Daily Archives: June 30, 2026

Imaam Ahmad bin Hambal (rahimahulla) Kupindura kuchoka kwa Bishr Haafi (rahimahulla)

Nkhani yotsatirayi ikuunikira kumvetsetsa kwakuya kwa dini ndi ma’rifat (kuzindikirika) ya Allah Talaa zomwe Allah Talaa adamudalitsa nazo Bishr Haafi (rahimahulla) zomwe zidachititsa kuti mpaka Imam Ahmad (rahimahulla) amutsanzire: M’nthawi ya Imaam Ahmad bin Hambal (rahimahulla) kunali dotolo wina yemwe ankatchedwa kuti Abdur Rahmaan At-Tabeeb. Ankathandiza Imaam Ahmad bin Hambal …

Read More »