Ma ubwino omwe munthu yemwe amakaswalira kunzikiti amapeza

1. Kupangira wudhu kunyumba komanso Kuyenda kupita kunzikiti ndi njira yokhululukidwa machimo ndikukwezedwa ulemelero.

عن أبي هريرة رضي الله عنه قال قال رسول الله صلى الله عليه وسلم من تطهر في بيته ثم مشى إلى بيت من بيوت الله ليقضي فريضة من فرائض الله كانت خطواته إحداهما تحط خطيئة والأخرى ترفع درجة (صحيح مسلم، الرقم: 666)

Sayyiduna Abu Hurairah (radhiyallahu anhu) akufotokoza kuti Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) adati: Munthu amene angapange wudhu kunyumba ndi Kuyenda wapansi kupita kunzikiti kuti akakwaniritse lamulo la Allah phanzi lirilonse lomwe angaponye amakhulukidwa machimo, ndipo phanzi lina lomwe angaponye adzakwezedwa ulemelero wake.

2. Omwe amabwera kunzikiti amatengedwa kuti ndi mulendo wa Allah.

عن عمرو بن ميمون عن عمر رضي الله عنه قال المساجد بيوت الله في الأرض وحق على المزور أن يكرم زائره (المصنف لابن أبي شيبة، الرقم: 35758)

Sayyiduna Amr bin Maimoon (rahimahullah) akulongosora kuti Umar (radhiyallahu anhu) adati: Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) adati: “mizikiti ndi nyumba za Allah padziko la pansi ndipo munthu aliyense amatenga udindo oyang’anira mlendo wake”.

3.Onse amene amapitapita kunzikiti amapatsidwa dzina loti “m’modzi wa omwe akukhala mnyumba ya Allah” komanso kapolo wapaderadera wa Allah.

عن أنس بن مالك رضي الله عنه قال سمعت رسول الله صلى الله عليه وسلم يقول إن عمار بيوت الله هم أهل الله عز وجل (مجمع الزوائد، الرقم: 2030)

Sayyiduna Anas (radhiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (sallallahu alaih wasallam)adati: anthu amene amabwerabwera kunzikiti okha ndi omwe ali akapolo apaderadera a Allah”.


[1] قال الهيثمي: رواه الطبراني في الأوسط وأبو يعلى والبزار وفيه صالح المري وهو ضعيف صالح ابن بشير ابن وادع المري بضم الميم وتشديد الراء أبو بشر البصري القاص الزاهد ضعيف من السابعة مات سنة اثنتين وسبعين وقيل بعدها (تقريب التهذيب صـ 271) عن أبي الدرداء رضي الله عنه قال سمعت رسول الله صلى الله عليه وسلم يقول المسجد بيت كل تقي وتكفل الله لمن كان المسجد بيته بالروح والرحمة والجواز على الصراط إلى رضوان الله إلى الجنة (الترغيب والترهيب، الرقم: 501) قال الهيثمي: رواه الطبراني في الكبير والأوسط والبزار وقال إسناده حسن وهو كما قال رحمه الله تعالى

Check Also

Masunnah Ochita Mumzikiti

27. Khalani mwaulemu ndi modekha pamene muli mumzikiti musakhale moiwala kulemekezeka kwa mzikiti. Anthu ena …