Chisilamu ndichipembedzo chomwe chili ndi ukhondo Kwambiri, chisilamu chimalimbikitsa ukhondo komanso kudziyeretsa m'magawo onse amoyo wamunthu,
Nabi (sallallahu alaih wasallam) adati:
الطهور شطر الإيمان
"Kudziyeretsa nditheka ya chikhulupiliro"
Read More »