Sahaabah

Nkhumbo lalikulu la Olemekezeka Saiid bin Zaid (Radhwiya Allaahu ‘anhu) lopereka Moyo Wake Munjira Ya Allah.

Mzinda wa Damasiko utagonjetsedwa ndi Asilamu, Abu Ubaidah (radhwiyallahu ‘anhu) mkulu wa asilikali achisilamu -anasankha Sa’iid bin Zaid (radhwiyallahu ‘anhu) kukhala kazembe wa mzinda wa Damasiko. Pambuyo pake Abu Ubaidah (Radhwiyallahu ‘anhu) adapitilira ndi gulu lake lankhondo kulowera ku Jordan. Atafika ku Yordan, anamanga msasa kumeneko ndi kuyamba kukonzekera zolimbana …

Read More »

Hazrat Sa’eed bin Zaid (Radhwiyallahu ‘anhu) Kuteteza maSwahaabah (Radhwiyallahu ‘anhum)

Nthawi ina Mughiirah bin Shu’bah (Radhwiyallahu ‘anhu) atakhala pamodzi ndi anthu ena mu Musjid ya ku Kufah, Sa’eed bun Zayd (radhwiyallahu ‘anhu) adalowa mu mzikiti. Mughiirah (Radhiyallahu ‘anhu) adamulonjera ndipo mwaulemu adamupempha kuti akhale pansi pa nsanja yomwe idali patsogolo pake. Patapita nthawi pang’ono, munthu wina wa ku Kufah adalowa …

Read More »

Hazrat Sa’iid bin Zaid (Radhwiyallahu ‘anhu) Apirira ku Mavuto Chifukwa Chachisilamu.

Hazrat Umar (radhwiyallahu ‘anhu) – munthu yemwe dzina lake loyera ndi njira yolemekezera chisilamu, ndipo changu cha imaani chinali chotere mpaka lero, patadutsa zaka 1300, anthu osakhulupirira amamuopabe,adali otchuka chifukwa chowazunza Asilamu (iyeyo) asanalowe Chisilamu. Adapitilizanso kufunafuna mipata yomupha Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam). Tsiku lina maquraish adasonkhana. …

Read More »

Dua ya Hazrat Said bin Zaid (Radhwiyallahu ‘anhu) Iyankhidwa

Nthawi ina, Arwa bint Uwais, neba wa Hazrat Said bin Zaid (Radhwiyallahu ‘anhu), adadza kwa Muhammad bin ‘Amr bin Hazm (Rahimahullah) ndi dandaulo lokhudza neba wake Hazrat Sa’eed bun Zaid (Radhwiyallahu ‘anhu). Ananena kuti adamanga khoma lake m’malo mwake ndipo adapempha Muhammad bin Amr (Rahimahullah) kuti apite kwa iye kuti …

Read More »

Sayyiduna Sa’iid Ibn Zaid (Radhwiyallahu ‘anhu) Ayikidwa m’gulu la Otenga nawo gawo pa nkhondo ya Badr

Nkhondo ya Badr isanayambike, Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) atamva kuti gulu la ochita malonda la Ma Quraish, lolemedwa ndi chuma chawo, lachoka ku Shaam (Syria) ndipo likubwerera ku Makkah Mukarramah, adatumiza Talhah bin Ubaidullah ndi Sa’iid radhwiyallahu anhuma kuti akasonkhanitse uthenga okhudza Gululi. Izi zidachitika masiku khumi Rasulullah (Swalla …

Read More »

Hazrat Abdur Rahmaan bin Auf (Radhiyallahu ‘anhu) Kusamalira akazi olemekezeka a Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wa sallam) paulendo wa Hajj

Rasulullah (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam) adati: “Ndithu, amene angadzasamalire akazi anga ndikadzamwalira, ndiye munthu owona ndi owopa Allah. Atamwalira Rasulullah (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam), Olemekezeka Abdur Rahmaan bun Auf (Radhwiyallahu ‘anhu) ankakhala myandikana ndi Azwaaj Mutahharaat (akazi olemekezeka a Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam)). …

Read More »

Sayyiduna ‘Abdur Rahmaan bin ‘Auf (Radhiyallahu ‘anhu) apatsidwa Udindo osankha Khalifah.

Pambuyo pake, Sayyiduna “Umar (radhiyallahu ‘anhu) adapanga Shura (gulu la akuluakulu omwe azipanga ziganizo) lokhala ndi ma Swahaabah asanu ndi mmodzi otsatirawa: Ali (radhiyallahu ‘anhu), ‘Uthmaan (radhiyallahu ‘anhu), Zubair (radhiyah ‘anhu) Sa’d (Radhiyallahu ‘anhu) ndi Abdur Rahmaan bun ‘Auf (radhiyallahu ‘anhu). Pankhani ya ma Sahaabah asanu ndi mmodziwa (Radhiyallahu ‘anhum), …

Read More »

Kuopa kwa Olemekezeka Abdur Rahman bin Auf (radhiyallahu ‘anhu) kufunsidwa

Naufal bin lyaas al Huzali (rahimahullah) adati: ‘Tikakhala pamodzi ndi Abdur Rahman bin Auf (Radhwiyallahu ‘anhu), ndi kukhala naye chifupi kodabwitsa kusangalatsirenji. Tsiku lina, anatitengera kunyumba kwake kuti tikadye, Titakhala pansi kuti tidye ndipo mbale ya chakudya ya nyama ndi mkate inaperekedwa pamaso pathu, iye adayamba kulira. Tidamufunsa: “Nchiyani chikukupangitsa …

Read More »

Kulandira Uthenga Wabwino Wamwayi Ndi Chikhululukiro M’maloto

Usiku wina, Hazrat Abdur Rahmaan bin Auf (Radhwiyallahu ‘anhu) adakomoka kwa nthawi yayitali chifukwa chakudwala kwake mpaka omwe anali pafupi naye adaganiza kuti mzimu wake wachoka. Anamuphimba ndi nsalu n’kuchokapo. Mkazi wake, Ummu Kulthum bint ‘Uqbah, nthawi yomweyo adapempha thandizo kwa Allah Ta’ala podekha ndi kuswali (monga talamulidwa kutero mu …

Read More »

Abdur Rahmaan bin Auf (Radhwiyallahu ‘anhu) agwiritsa ntchito Chuma chake pa nkhondo ya Tabuk.

Pamene Allah Ta’ala ankamulamula Rasulullah (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) kuti anyamuke ulendo wa ku Tabuk, ma Swahaabah ambiri adalibe kalikonse panthawiyo zoti athandizikirw kuyende ulendo wautali ndi wotopetsa, makamaka pamene ankayembekezera kukumana ndi gulu lankhondo lachiroma pankhondo yomwe inali ndi zida zokwanira komanso adalipo ambiri. Choncho pofuna kusonkhanitsa pamodzi ndi …

Read More »