Miswar bin Makhramah (Radhwiyallahuanhu) akuti: Abdur Rahmaan bun Auf (Radhwiyallahu ‘anhu) nthawi ina adagulitsa munda wa mpesa kwa Uthman (Radhwiyallahu ‘anhu) pamtengo wa ma dinari zikwi makumi anayi (40,000). Abdur Rahmaan (Radhwiya Allaahu ‘anhu) atalandira ndalamazo kuchokera kwa Uthmaan (Radhwiyallahu ‘anhu), nthawi yomweyo adazigawa kwa akazi odalitsika a Mtumiki (Swalla …
Read More »Abdur-Rahman bin Awf (Radhwiyallahu ‘anhu) amatsogolera Swalaah
Paulendo wa Tabuuk, ma Swahaabah (Radhwiyallahu ‘anhum) adali pa ulendo ndi Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam). Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) adachoka kwa ma Swahaabah (Radhwiyallahu ‘anhum) kuti apite kukazithandiza. Popeza kuti nthawi ya Swalah ya Fajr sidali yochuluka, ndipo ma Swahaabah (Radhwiyallahu ‘anhum) ankaopa kuti nthawi itha kutha, sadamudikire …
Read More »Olemekezeka Abdur Rahman bin Auf (Radhwiyallahu ‘anhu) ndi mmodzi mwa Asilamu opambana.
Nthawi ina Rasulullah (Swalla-Allaahu ‘alayhi wasallam) adamufunsa Busrah bint Safwan (Radhwiya-Allahu ‘anha) kuti ndi ndani amene ankafuna kukwatira mphwake, Umm Kulthuom bint Uqbah. Adamufotokozera mayina a anthu ochepa omwe adamfunsira mphwakeyo, ndipo adamuwuzanso kuti mwa anthu omwe adamfunsira mphwakeyo ndi Abdur Rahman bin Auf (Radhwiyallahu ‘anhu). Zitatero, Mtumiki (Swalla-Allaahu ‘alayhi …
Read More »Olemekezeka Talhah (Radhwiyallahu ‘anhu pa Nkhondo ya Uhud
Pankhani ya kupirira kwa Talha (Radhwiyallahu ‘anhu) pankhondo ya Uhud, Sa’d bin Abi Waqqaas (Radhwiyallahu ‘anhu) adanena izi: Allah Ta’ala amuchitire chifundo Talha. Mosakayikira, mwa ife tonse, adamuthandiza kwambiri Mtumiki (Swallallaahu ‘alayhi wa wasallam) pa tsiku la Uhud. Kenako Sa’d (Radhwiyallahu ‘anhu) adafunsidwa: “Tifotokozere momwe (adamuthandizira kwambiri Mtumiki (Swallallaahu ‘alayhi …
Read More »Mlamu wa Rasulullah (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wa sallam)
Olemekezeka Talhah (Radhwiyallahu ‘anhu) adakwatira akazi okwana anayi. Aliyense mwa akazi ake anayi anali pachibale ndi m’modzi mwa akazi olemekezeka a Mtumiki (Swallallaahu ‘alayhi waaalihi wasallam). Ndichifukwa chake Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam) adamuuza kuti: “(Ndiwe) mlamu wanga padziko lapansi ndi tsiku lotsiriza (kutanthauza kuti udzakhalanso mlamu wanga …
Read More »Kuwolowa kwambiri manja kwa Talhah (Radhwiyallahu ‘anhu)
Mkazi wa Talhah (Radhwiyallahu ‘anha), Su’da bint ‘Awf al-Muriyyah anakambapo izi zokhudza mwamuna wake Talhah (Radhwiyallahu ‘anhu): “Tsiku lina Talha analowa m’nyumba ali okhumudwa. Chavuta ndi chiyani? Kodi ndalakwitsa penapake mchifukwa ndikuwona kuti mukuonetsa kukhumudwa? Chonde ndiuzeni kuti ndithe kuchotsa kukhumudwa kwanu. Iye adayankha, “Ayi, siunandilakwire chilichonse, ndipo ndithudi, ndiwe …
Read More »Kulandira dzina la Al-Fayyadh kuchokera kwa Mtumiki swallallahu alaihi wasallam
Rasulullah (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam) adampatsa olemekezeka Talhah (radhwiyallahu ‘anhu) dzina loti Al-Fayyaadh (munthu owolowa manja kwambiri) kangapo. Pansipa pali nkhani imodzi yotere: Pankhondo ya Zi Qarad, Rasulullah (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam) adadutsa pachitsime cha Baisaan. Madzi a m’chitsimechi ankadziwika kuti ndi anchere. Rasulullah (Swalla Allaahu …
Read More »Olemekezeka Talhah (Radhwiyallahu ‘anhu) Kukwaniritsa Lonjezo Lake
Olemekezeka Talhah (Radhwiyallaahu ‘anhu) akuti: Ma Swahaabah (Radhwiya Allahu ‘anhum) adauza munthu wina okhala kumudzi kuti: “Pita ukafunse kwa Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) kuti Allah Ta’ala akunena za ndani (m’ndime yotsatira ya Quraan Majeed)” (ma Sahaabah) ndi amene adakwaniritsa lonjezo lawo (ndi Allah Ta’ala lokhala okhazikika pankhondo okonzeka kupereka …
Read More »Olemekezeka Talhah (Radhiyallahu ‘anhu) pa Nkhondo ya Uhud
Olemekezeka Jaabir bin Abdillah (Radhwiya Allaahu ‘anhu) adati: Pa tsiku la nkhkndo ya Uhud, pamene ma Swahaabah adayamba kuthawa kunkhondo, Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) adasiidwa yekha pamalo ena ndi ma Swahaaba khumi ndi awiri okha.) Ma mushrikiin atapita kwa Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) ndi ma Swahaabah khumi ndi …
Read More »Chisilamu cha Olemekezeka Talhah bin Ubaidillah (Radhwiyallahu ‘anhu)
Tsiku lomwe sayyiduna Abu Bakr Siddeeq (Radhwiyallahu ‘anhu) adalowa Chisilamu, adayamba kuyitanira anthu ku Chisilamu, Allah Ta’ala adamupanga kukhala njira ya ma Swahaabah (radhwiyallahu ‘anhun) ambiri kulowa Chisilamu. Mwa ma Swahaabah amene adalowa Chisilamu kudzera mwa Abu Bakr Siddeeq (radhwiyallahu ‘anhu) anali Talhah bin Ubaidillah (radhwiyallahu ‘anhu). Talhah (radhwiyallahu ‘anhu) …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu