Mazhab anayi Kuyambira nthawi ya Sayyiduna Rasulullah, ma Swahaabah, Taabi’een ndi zaka mazana zotsatira, akazi ankalamulidwa kuswali m’njira yosiyana ndi Swalaah ya amuna m’magawo ena za swalah. Madhabu onse anayi (omwe ndi Hanafi, Maliki, Shafi’i ndi Hambali) onse amagwirizana pa mfundo yakuti Swalaah ya akazi imasiyana ndi Swalaah ya amuna …
Read More »Kapempheredwe ka Azimayi
Chilichonse cha chipembedzo cha Chisilamu chokhudzana ndi akazi chimakhanzikika pa kukhala odzichepetsa komanso wamanyazi. Pachifukwa ichi ndi pamene Chisilamu chikulamula amayi kuti azikhala m’nyumba zawo, kukhala obisika kwa amuna achilendo, komanso kuti asachoke m’nyumba zawo popanda chifukwa chenicheni pa Sharia. M’mene mkazi walamulidwira kuswali Swalah yake – kuyambira pa chovala …
Read More »Sunna Za Msikiti
37. Ulumikizitseni mtima wanu nthawi zonse ndiku mzikiti. Mwachitsanzo pamene mukuchoka mumzikiti pomwe mwatsiriza swalah yanu, pangani niya kuti mubweranso kumzikitiko paswala yotsatirayo ndipo idikireni swalayo ndimtima onse.[1] عن أبي هريرة رضي الله عنه أن رسول الله صلى الله عليه وسلم قال ألا أدلكم على ما يمحو الله به الخطايا …
Read More »Sunna Za Msikiti
34. Kutha kwa Adhana, ngati sudapemphere swalah, usatuluke mumzikiti pokhapokha patakhala zifukwa zomveka bwino.[1] عن أبي الشعثاء قال كنا قعودا في المسجد مع أبي هريرة رضي الله عنه فأذن المؤذن فقام رجل من المسجد يمشي فأتبعه أبو هريرة رضي الله عنه بصره حتى خرج من المسجد فقال أبو هريرة رضي …
Read More »Masunnah Ochita Mumzikiti
31. Kupatula kupita kumzikiti kukapemphera, ngati kuli mtsonkhano omwe ukupangidwira mumzikiti, mukuyenera kupanga niya kuti mukupita kumzikiti kukaphunzira za Dini. Ngati wina angakwanitse kuphunzitsa dini choncho akuyenera kupanga niya kuti akubwera kumzikiti kukaphunzitsa dini. عن أبي هريرة رضي الله عنه قال سمعت رسول الله صلى الله عليه وسلم يقول من …
Read More »Masunnah Ochita Mumzikiti
27. Khalani mwaulemu ndi modekha pamene muli mumzikiti musakhale moiwala kulemekezeka kwa mzikiti. Anthu ena pamene akudikilira swalah kuti ichitike amaseweretsa zovala zawo kapena kusoweretsa mafoni. Kumeneku ndikuphwanya kulemekezeka ndi ulemelero wa mnzikiti.[1] 28. Thandizirani poupanga mzikiti kuti ukhale waukhondo nthawi zonse.[2] عن أبي سعيد الخدري رضي الله عنه قال …
Read More »Masunnah Ochita Mumzikiti
26 Osaipitsira mumzikiti. mwachitsanzo kulavulira mumzikiti kapena kumina mumzikiti mpaka zoipazo maminawo kapena malovuwo mkugwera pansi munzikiti.[1] عن أبي ذر رضي الله عنه قال قال رسول الله صلى الله عليه وسلم عرضت علي أعمال أمتي حسنها وسيئها فوجدت في محاسن أعمالها الأذى يماط عن الطريق ووجدت في مساوئ أعمالها النخاعة …
Read More »Masunnah Ochita Mumzikiti
24. Sizili zoloredwa kumuchotsa munthu pamalo ake mumzikiti cholinga choti akhalepo wina.
Olemekezeka Ibnu Umar (radhwiyallah anhu) akunena kuti Mtumiki (salallah alayhi wasallama) adaletsa kuchotsedwa munthu wina pamalo ake ndikuti mumthu wina akhale pamalo ake. Choncho anthu akhoze malo oti akhale munthu amene (wabwera kumeneyo ngati zili zotheka kumupangira maloko).
Read More »Masunnah Ochita Mumzikiti
20. Osaimika swalah mumzikiti pa malo amene ungawatchingire anthu ena kudutsa mwaufulu. Mwachitsanzo kupemphera swalah pamalo polowera zimene zingapangitse ena kuti asadutse.
Olemekezeka Ibn Umar (radhiyallahu anhuma) akusimba kuti Mtumiki (sallallahu alayhi wasallama) adaletsa kupemphera swalah malo okwana asanu ndi awiri (ndipo amodzi mwamalowo) ndimalo odutsapo anthu.
Read More »Masunnah Ochita Mumzikiti
17. Osakangana ndiwina aliyense mumzikiti kumeneko ndikuonetsera kunyoza malo olemekezeka amzikiti.[1] 18. Ndipo ndizabwino kwambiri kuti musaupange mnzikiti kukhala njira yanu yodutsira popita tsidya lina.[2] عن ابن عمر رضي الله عنهما عن رسول الله صلى الله عليه وسلم قال خصال لا تنبغي في المسجد لا يتخذ طريقا ولا يشهر فيه سلاح …
Read More »