Sayyiduna Haani (rahimahullah), kapolo womasulidwa wa Sayyiduna “Uthmaan (radhiyallahu ‘anhu), akunena kuti: Hazrat ‘Uthmaan (radhiyallahu ‘anhu) ankati akayima pamanda, ankalira kwambiri moti ndevu zake zinkanyowa ndi misozi yake. Wina adamufunsa kuti: “Timakuwona kuti ukakumbukira Jannah ndi Jahanmum kapena kukambidwa za izo, siumakhudzidwa kwambiri mpaka kuyamba kulira, pomwe ukayima pamanda timakuona …
Read More »Kutsatira Njira Yofewa ndi Yodekha Pochita zinthu ndi Anthu:
“Ataa bin Farrookh (rahimahullah) akufotokoza motere: Tsiku lina lake ‘Uthmaan (radhwiyallaahu ‘anhu) adagula malo kwa munthu wina. Atagula malowa ‘Uthmaan (radhwiyallahu ‘anhu) adadikira kuti munthuyo adzatenge ndalama zake. Komabe, munthuyo sanabwere. ‘Uthmaan (radhiyallahu ‘anhu) adakumana ndi munthuyo pambuyo pake ndipo adamufunsa: “Bwanji sunabwere kudzatenga ndalama zako?” Bamboyo anayankha. “Chomwe chinandipangitsa …
Read More »Hayaa ya Hazrat ‘Uthmaan (Radhiyallahu ‘anhu)
Hazrat Aaishah (radhiya allahu ‘anha) akusimba motere: Nthawi ina, Mtumiki (swalla allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam) anali atagona kunyumba kwanga ndipo thupi lake linasunthidwa pang’ono kuchokera kudera la ntchafu zake zodalitsika kapena ntchafu yake yodalitsika, ngakhale ntchafu zodalitsidwa ndi shins zidakutidwa ndi lungi lake. Panthawi imeneyo, Abu Bakr (radhiyallahu ‘anhu) …
Read More »Nkhani Zabwino Za Jannah
Sayyiduna Abu Muusa (Radhwiya Allaahu ‘anhu) akufotokoza motere: Tsiku lina ndidali limodzi ndiMtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) mu umodzi mwa minda ya zipatso zaku Madinah Munawwarah pamene munthu wina adadza napempha chilorezo cholowa m’mundawu, atamva pempho la munthuyo, Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) anandiuza. “Mlole alowe ndikumuwuza nkhani yabwino yokhala …
Read More »Msilamu Woyamba Kuchita Hijrah (kusamuka) ndi Banja Lake
Olemekezeka Anas (radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Uthmaan (radhwiyallahu anhu) adanyamuka kupita ku Abyssinia, kusamuka ndi mkazi wake olemekezeka, Bibi Ruqayyah (radhwiyallahu anha), mwana wamkazi wodalitsika wa Rasulullah (swallallaahu alaih wasallam). Nkhani zokhudza momwe amakhalira zidachedwa, choncho Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) adali ndi nkhawa ndipo amatuluka ku Makka Mukarramah kufuna kudziwa …
Read More »Kugula Chitsime ku Jannah
Pamene Masahaabah (radhiyallahu ‘anhum) adasamukira ku Madinah Munawwarah, madzi omwe adawapeza kumeneko adali ovuta kwa iwo kumwa popeza adali anchere. Komabe, padali Myuda wina yemwe amakhala ku Madinah Munawaarah yemwe adali ndi chitsime chamadzi okoma otchedwa Ruumah, ndipo ankagulitsa madzi a pachitsime chakewo kwa maswahaabah (radhiyallahu ‘anhum). Mtumiki (swallallaahu ‘alayhi …
Read More »Sayyiduna Umar (Radhiyallahu ‘anhu) Kulamula Zabwino Panthawi Yotsiriza (yamoyo wake)
M’mawa wa tsiku limene Sayyiduna Umar (Radhwiya Allahu ‘anhu) adabayidwa, mnyamata wina adamuyendera nati kwa iye: “Ameer-ul-Mu’mineen! Sangalalani ndi nkhani yabwino yochokera kwa Allah Ta’alal, Inu ndinu Sahaabi wa Mtumiki (Swallallaahu ‘alayhi wasallam) Ndipo inu muli m’gulu la anthu amene adalandira Chisilamu m’masiku oyambirira, ndipo mudasankhidwa kukhala Khalifa ndipo mudachita …
Read More »Hazrat Umar (radhwiyallahu anhu) Kufuna kuyikidwa pafupi ndi Rasulullah (swallallaahu alaih wasallam)
Pakati pa mphindi zomaliza pambuyo pa Hazrat Umar (radhiliyalahlah ‘Ahu) adaphedwa mwangozi, Anatumiza mwana wake, Hazrat Abdullah Bin Umar (radhwiyallahu ‘Anhuma), kunyumba kwa Hazrat Aaishah (radhiyallahu ‘ahha). Hazrat Umar (Radhiyallahu anhu adamulangiza iye kuti ukamuuze kuti Umar akupereka Salaam. Usakanene kuti Amiirul muuminiin popeza kuyambira lero sindidzaitanidwanso …
Read More »Kudzichepetsa kwa Sayyiduna Umar (Radhwiyallahu ‘anhu)
Olemekezeka Miswar bin Makhramah (radhwiyallahu ‘anhu) akusimba kuti pamene Umar (radhwiyallahu ‘anhu) anabayidwa, iye anayamba kumva chisoni ndi kukhala ndi nkhawa kwambiri kuudandaulira ummah. Ibnu Abbaas (radhwiyallahu ‘anhu) adamtonthoza nati: “Oh Ameer-ul-Mu’mineen! Palibe chifukwa chodandaulira. Mudakhala pamodzi ndi Mtumiki (swallallaahu ‘alayhi wasallam) ndipo mudakwaniritsa ma ufulu ake onse . Ubwenzi …
Read More »Ulemu wa Umar (radhwiyallahu ‘anhu) kwa Abu Bakr (radhwiyallahu ‘anhu)
Hazrat Umar (radhiyallahu anhu) nthawi zonse ankavomereza udindo wapamwamba wa Hazrat Abu Bakr (radhwiyallahu ‘anhu) ndipo sankadzitenga ngati iye ndi wofanana ndi Abu Bakr (radhwiyallahu ‘anhu). Ulendo wina gulu la anthu linamutamanda Umar (radhwiyallahu ‘anhu) ponena kuti: “Ndikulumbirira kwa Allah! Sitinaonepo munthu wolungama, wonena zoona, ndi wokhwimitsa zinthu kwambiri kwa …
Read More »