Sahaabah

Kukhudzika kwa Sayyiduna Umar (Radhwiyallahu ‘anhu) pa Swalaah

M’mawa womwe Umar (radhwiya allaahu ‘anhu) adabayidwa, Olemekedzeka Miswar bin Makhramah (radhwiyallahu ‘anhu) adadza kudzamuona. Polowa mnyumba adapeza Umar (radhwiyallahu ‘anhu) atafunditsidwa ndi ndi nsalu ali chikomokere. Olemekezeka Miswar (radhwiyallahu ‘anhu) adafunsa anthu omwe adalipo pamenepo kuti, “Ali bwanji?” Iwo anayankha kuti: “Ali chikomokere monga mukuwoneramu.” Chifukwa panalibe nthawi yochuluka …

Read More »

Hazrat Umar (radhwiyallahu ‘anhu) Kulemekeza Azwaaj-e-Mutahharaat (radhwiyallahu ‘anhunna)

Olemekezeka Aslam (rahimahullah), kapolo wa Sayyiduna Umar (radhwiyallahu anhu), akufotokoza kuti Umar (radhwiyallahu ‘anhu) anali ndi mbale zisanu ndi zinayi zomwe zidasungidwa kuti azitumizira mphatso kwa Azwaa-e-Mutwahharaat (akazi olemekezeka a Mtumiki (Swallallaahu ‘alayhi wasallam) di amayi a Ummah). Olemekezeka Aslam (rahimahuliah) adanena kuti nthawi iliyonse kukafika chakudya chokoma, zipatso kapena …

Read More »

Kusamalitsa pa Chuma cha Anthu

Kusamalitsa komwe olemekezeka Umar (radhwiyallahu ‘anhu)adachita pa kagwiritsidwe ntchito ka chuma cha anthu kunalidi kosasimbika. Nthawi ina, musk (mtundu wa mafuta onunkhira) anabweretsedwa kuchokera ku Bahrain. Ngati chuma cha anthu onse, Umar (radhwiya allaahu ‘anhu) adati: “Ndikulumbirira kwa Allah! Ndikufuna nditapeza munthu wodziwa kuyeza zinthu kuti andipimire mafutawa kuti ndiwagawe …

Read More »

Olemekezeka Umar (radhwiyallahu ‘anhu) adzikumbutsa za Kuyankha mafunso pa Tsiku Lachiweruzo

Ngakhale Allah Ta’ala adamudalitsa Umar (radhwiyallahu ‘anhu) pokhala m’gulu la anthu khumi omwe adalonjezedwa kukalowa ku Jannah ali padziko lino lapansi, ndipo ngakhale adali khalifah wachiwiri wa Chisilamu, adali wodzichepetsa kwambiri ndikuwopa kuyankha mafunso pamaso pa Allah Ta’ala pa tsiku la Qiyaamah. Zikunenedwa kuti nthawi ina, Olemekezeka Umar (radhwiyallahu ‘anhu) …

Read More »

Hazrat Ali (radhwiyallaahu ‘anhu) Akufuna Kukumana ndi Allah Ta’ala ndi zochita za Hazrat Umar (radhwiyallaahu ‘anhu)

Olemekezeka Abdullah bin Abbaas (radhwiyallaahu ‘anhuma) akunena kuti: Ndinalipo pa nthawi yomwe mtembo wa Umar (radhwiyallahu ‘anhu) unkaikidwa pa Jeneza ataphedwa. Anthu anayamba kuthamangira pamene padali thupi lake. Pamene ankayembekezera kuti mtembo wake utulutsidwe ndi kuikidwa m’manda, iwo ankawerenga durood kumfunira zabwino Rasulullah (swallallaahu ‘alayhi wasallam) ndikumamupemphera Umar (radhwiyallahu ‘anhu). …

Read More »

Chisangalalo cha Hazrat Umar (Radhiyallahu ‘anhu)

Olemekezeka Umar (Radhwiyallaahu ‘anhu) adanenapo nthawi ina kwa olemekezeka Abbaas (Radhwiyallahu ‘anhu) (amalume a Rasulullah (Swallallaahu ‘alayhi wasallam)) kuti: “Ndidakondwera ndi Chisilamu chanu kuposa Chisilamu cha abambo anga chifukwa Chisilamu chanu chidabweretsa chisangalaro chochuluka kwa Rasulullah swallallahu ‘alaihi wasallam) kuposa Chisilamu cha bambo anga. (Sharhu Ma’aanil Aathaar 3/321)

Read More »

Hazrat Abu Bakr – manthu cha Ubwino ndi Chifundo

Tsiku lina Rasulullah (swallallaahu ‘alayhi wasallam) adafunsa kwa ma Swahaabah (radhwiyallahu “anhum) kuti: “Ndani mwa inu amene akusala kudya lero?” Hazrat Abu Bakr (radhiyallahu anhu) adayankha: “Lero ndasala. Kenako Nabiy (swallallaahu ‘alayhi wasallam) adafunsa. “Ndani mwa inu amene wayendera munthu wodwala lero?” Harrat Abu Bakr (radhiyallahu ‘anhu) adayankha: “Lero ndayendera …

Read More »

Munthu Woyamba wa Ummah uwu kukalowa ku Jannah

M’ Hadith ya yodaliysika, Rasulullah (swallallaahu ‘alayhi wasallam) adalongosora kuti Ummah wake udzalowa ku Jannah pamaso pa ma Ummah ena onse, ndipo kuchokera mu Ummah wake wonse, Hazrat Abu Bakr (radhwiyallahu ‘anhu) adzakhala munthu woyamba kulowa ku Jannah pambuyo pake. Mtumiki (swallallaahu ‘alayhi wasallam) adati: “Hazrat Jibreel (‘alaihis salaam) adaonekera …

Read More »

Hazrat Abu Bakr (Radhwiyallahu ‘anhu) akhala Wokonzeka kupereka nsembe ya china Chilichonse

Mtumiki (Swallallaahu ‘alayhi wa sallam) Pankhondo ya Badr, mwana wa Abu Bakr Siddeeq (radhwiyallahu anhu) Hazrat Abdur Rahmaan (Radhwiyallahu ‘anhu), anamenya nawo mbali ya okanira poti iye adali asadakhulupirirebe Chisilamu. Pambuyo pake, atalowa Chisilamu, ali chikhalire pansi ndi bambo ake, Hazrat Abu Bakr Siddeeq (Radhwiyallahu “anhu), adati: “E, inu abambo …

Read More »