Tafseer Ya Surah Qadr

بِسمِ اللّٰـهِ الرَّحمٰنِ الرَّحيمِ اِنَّا أَنزَلنٰهُ فى لَيْلَةِ القَدْرِ ﴿١﴾ وَما أَدرىٰكَ ما لَيلَةُ القَدرِ ﴿٢﴾ لَيلَةُ القَدرِ خَيرٌ مِن أَلفِ شَهرٍ ﴿٣﴾ تَنَزَّلُ المَلـٰئِكَةُ وَالرّوحُ فيها بِإِذنِ رَبِّهِم مِن كُلِّ أَمرٍ ﴿٤﴾ سَلـٰمٌ هِىَ حَتّىٰ مَطلَعِ الفَجرِ ﴿٥﴾ Ndithudi, Tayimvumbulutsa Qur’an mu usiku wa Qadr (olemekezeka kwambiri). Ndipo chingakudziwitse nchiyani za usiku olemekezeka kwambiriwu (Usiku wa qadar). Usiku …

Read More »

Kupeza nawo chiombolo cha Mtumiki sallallahu alaih wasallam

عن رويفع بن الثابت قال: قال رسول الله صلى الله عليه وسلم: من صلى على محمد وقال: اللهم أنزله المقعد المقرب عندك يوم القيامة، وجبت له شفاعتي (المعجم الكبرى للطبراني، الرقم: 4480 ،وإسناده حسن كما في مجمع الزوائد، الرقم: 17304) Olemekezeka Ruwaifidh  (radhiyallahu anhu) akufotokoza kuti, Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) …

Read More »

Kuonjezereka kwa ma riziqi

عن سهل بن سعد رضي الله عنه قال: جاء رجل إلى النبي صلى الله عليه وسلم فشكا إليه الفقر وضيق العيش أو المعاش فقال له رسول الله صلى الله عليه وسلم: إذا دخلت منزلك فسلم إن كان فيه أحد أو لم يكن فيه أحد ثم سلم علي واقرأ قل هو …

Read More »

Mawu A Iqaamah Komanso Njira Ya Sunnat Yopangira Iqaamah

6. Tembenuzirani nkhope yanu kumanja pamene mukunena kuti: Hayya alas swalah ndiponso kumanzere pamene mukunena kuti: Hayya alaal falaah.[1] 7. Pamene Iqaamah yachitidwa musakhale otangwanika ndikupemphera swalati ya sunnah. Choncho kungotha iqaamah pompopompo yambani kupemphera ya faradh.[2] عن أبي هريرة رضي الله عنه عن النبي صلى الله عليه وسلم قال …

Read More »

Sawabu zapaderadera ukawerenga Durood ka 100

عن أبي هريرة رضي الله عنه عن النبي صلى الله عليه وسلم قال من صلى علي عشرا صلى الله عليه مئة ومن صلى علي مئة صلى الله عليه ألفا ومن زاد صبابة وشوقا كنت له شفيعا وشهيدا يوم القيامة (أخرجه أبو موسى المديني بسند قال الشيخ مغلطاى لا بأس به، …

Read More »

Mawu A Iqaamah Komanso Njira Ya Sunnat Yopangira Iqaamah

3. Pangani adhaan mofulumira poyankhula komanso motsitsa mawu.

Olemekezeka Jaabir (Radiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (salallahu alayhi wasallama (adamuuza Bilal (radhiyallahu anhu): Pamene ukupanga adhaan panga pang´onopang´ono (komanso uziima pambuyo powerenga mnzere uliwonse) Komano pamene ukupanga iqaamah ukuyenera upange mwachanguchangu."

Read More »

Kupeza nawo duwa yapaderadera ya Angelo

Sayyiduna Aamir bin Rabeeah (radhiyallahu anhu) akulongosora kuti Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) adati: Amene angandifunire zabwino angero amamufunira zabwino munthu ameneyo (amampangira duwa) kwa nthawi yomwe iye angamamfunire zabwino Mtumiki (sallallahu alaih wasallam), kotero chisankho chili ndi iye kuchulukitsa duruud kapena kuchepetsa.

Read More »

Mawu A Iqaamah Komanso Njira Ya Sunnat Yopangira Iqaamah

1. Mawu a Iqaamah ndichimodzimodzi ndi azaana. Koma popanga iqaamah mukuyenera kunena kamodzikamodzi kupatula mawu onena kuti قد قامت الصلاة (Qadi qaamatis swalaah) mukuyenera kunena kawiri. Choncho mukatsiriza mawu oti Hayya alaal falaah mudzanena kuti: قَدْ قَامَتِ الصَّلَاةْ قَدْ قَامَتِ الصَّلَاةْ Qad qaamatis swalat, qad qaamatis swalaah (Swalah yaima swalah …

Read More »