عن سهل بن سعد رضي الله عنه قال: جاء رجل إلى النبي صلى الله عليه وسلم فشكا إليه الفقر وضيق العيش أو المعاش فقال له رسول الله صلى الله عليه وسلم: إذا دخلت منزلك فسلم إن كان فيه أحد أو لم يكن فيه أحد ثم سلم علي واقرأ قل هو …
Read More »Kuyankha Mawu A Iqaamah
Yankhani iqaama mofanana ngati mmene mumayankhira adhaan. Komabe pamene mukuyankha mawu awa قَدْ قَامَتِ الصَّلاَهْ (qad qaamatis salaah) mudzanena kuti:
Read More »Sawabu zofanana ndikupereka sadaqah ukawerenga Duruud
Olemekezeka Abu Sa'eed khudri (radhiyallahu anhu) akufotokoza kuti Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) adati, "Msilamu amene alibe kena kalikonse kuti apereke sadaqah adziwerenga duruud iyi mkatikati mwa duwa yake popeza idzampezetsa iyeyo sawabu zoti wapeleka sadaqah ndikumuyeretsa ku machimo.
Read More »Mawu A Iqaamah Komanso Njira Ya Sunnat Yopangira Iqaamah
6. Tembenuzirani nkhope yanu kumanja pamene mukunena kuti: Hayya alas swalah ndiponso kumanzere pamene mukunena kuti: Hayya alaal falaah.[1] 7. Pamene Iqaamah yachitidwa musakhale otangwanika ndikupemphera swalati ya sunnah. Choncho kungotha iqaamah pompopompo yambani kupemphera ya faradh.[2] عن أبي هريرة رضي الله عنه عن النبي صلى الله عليه وسلم قال …
Read More »Sawabu zapaderadera ukawerenga Durood ka 100
عن أبي هريرة رضي الله عنه عن النبي صلى الله عليه وسلم قال من صلى علي عشرا صلى الله عليه مئة ومن صلى علي مئة صلى الله عليه ألفا ومن زاد صبابة وشوقا كنت له شفيعا وشهيدا يوم القيامة (أخرجه أبو موسى المديني بسند قال الشيخ مغلطاى لا بأس به، …
Read More »Mawu A Iqaamah Komanso Njira Ya Sunnat Yopangira Iqaamah
3. Pangani adhaan mofulumira poyankhula komanso motsitsa mawu.
Olemekezeka Jaabir (Radiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (salallahu alayhi wasallama (adamuuza Bilal (radhiyallahu anhu): Pamene ukupanga adhaan panga pang´onopang´ono (komanso uziima pambuyo powerenga mnzere uliwonse) Komano pamene ukupanga iqaamah ukuyenera upange mwachanguchangu."
Read More »Kupeza nawo duwa yapaderadera ya Angelo
Sayyiduna Aamir bin Rabeeah (radhiyallahu anhu) akulongosora kuti Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) adati: Amene angandifunire zabwino angero amamufunira zabwino munthu ameneyo (amampangira duwa) kwa nthawi yomwe iye angamamfunire zabwino Mtumiki (sallallahu alaih wasallam), kotero chisankho chili ndi iye kuchulukitsa duruud kapena kuchepetsa.
Read More »Mawu A Iqaamah Komanso Njira Ya Sunnat Yopangira Iqaamah
1. Mawu a Iqaamah ndichimodzimodzi ndi azaana. Koma popanga iqaamah mukuyenera kunena kamodzikamodzi kupatula mawu onena kuti قد قامت الصلاة (Qadi qaamatis swalaah) mukuyenera kunena kawiri. Choncho mukatsiriza mawu oti Hayya alaal falaah mudzanena kuti: قَدْ قَامَتِ الصَّلَاةْ قَدْ قَامَتِ الصَّلَاةْ Qad qaamatis swalat, qad qaamatis swalaah (Swalah yaima swalah …
Read More »Sawabu zomwe munthu amapeza akawerenga Durood
عن أنس بن مالك قال: قال رسول الله صلى الله عليه وسلم: من ذكرت عنده فليصل علي فإنه من صلى علي مرة صلي عليه عشرا (المعجم الأوسط للطبراني، الرقم: 2767، ورجاله رجال الصحيح كما في القول البديع صـ 237) Olemekezeka Anas bin Maalik (radhiyallahu anhu) akufotokoza kuti Mtumiki (sallallahu alaih …
Read More »Duwa Yonena Panthawi Ya Adhaana Ya Maghreb
Werengani duwa iyi pamene ikuchitika azaana ya maghreb kapena kutha kwa azaana yamaghreb.[1] اَللّٰهُمَّ إِنَّ هٰذَا إِقْبَالُ لَيْلِكَ وَإِدْبَارُ نَهَارِكَ وَأَصْوَاتُ دُعَاتِكَ فَاغْفِرْ لِيْ Oh Allah, Uku ndikufika kwa usiku ndiponso kuchoka kwa Usana ndiponso awa ndimawu oitana a akapolo anu (mamuadhin) choncho ndikhululukireni machimo anga. عن أم سلمة رضي …
Read More »