Chisilamu ndi njira yokwanira komanso yangwiro ya moyo yomwe yaganizira zosowa zonse za munthu. Sizinangosonyeza njira ya mtendere m’moyo wa munthu, komanso zasonyeza mmene tingasonyezere chikondi ndi mtendere munthu akamwalira. Choncho Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) adausonyezera Ummah momwe ungatonthozere ndi kuwapepesa ofedwa amene ali m’masautso. Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) adati: …
Read More »Sayyiduna Sa’iid Ibn Zaid (Radhwiyallahu ‘anhu) Ayikidwa m’gulu la Otenga nawo gawo pa nkhondo ya Badr
Nkhondo ya Badr isanayambike, Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) atamva kuti gulu la ochita malonda la Ma Quraish, lolemedwa ndi chuma chawo, lachoka ku Shaam (Syria) ndipo likubwerera ku Makkah Mukarramah, adatumiza Talhah bin Ubaidullah ndi Sa’iid radhwiyallahu anhuma kuti akasonkhanitse uthenga okhudza Gululi. Izi zidachitika masiku khumi Rasulullah (Swalla …
Read More »Maduwa Oyenera Kupanga Ukakamuona Odwala
Dua Yoyamba لا يَأْسَ طَهُورٌ إِنْ شَاءَ الله Palibe chifukwa chodera nkhawa, insha-Allah kudzera m’matendawa, muyeretsedwa. (i.e. Palibenso chifukwa chilichonse choti mude nkhawa kapena kuchita mantha. Mukungoyeretsedwa ku Uzimu, mukuyeretsedwa ku machimo anu, ndipo kuthupi, thupi lanu likuyeretsedwa ku poizoni. Choncho, pamene matenda abwera kwa inu ngati chifundo chobisika kumbali …
Read More »Hazrat Abdur Rahmaan bin Auf (Radhiyallahu ‘anhu) Kusamalira akazi olemekezeka a Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wa sallam) paulendo wa Hajj
Rasulullah (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam) adati: “Ndithu, amene angadzasamalire akazi anga ndikadzamwalira, ndiye munthu owona ndi owopa Allah. Atamwalira Rasulullah (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam), Olemekezeka Abdur Rahmaan bun Auf (Radhwiyallahu ‘anhu) ankakhala myandikana ndi Azwaaj Mutahharaat (akazi olemekezeka a Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam)). …
Read More »Ana Olungama – Cholowa Cha Tsiku Lachiweluzo
Zina mwa zabwino zamtengo wapatali za Allah pa munthu ndi mdalitso okhala ndi ana. Mdalitso okhala ndi ana ndi ena mwa Ni’ma yapadera ya Allah, zomwe zatchuridwa mu Quraan Majiid. Allah Akunena: وَاللَّهُ جَعَلَ لَكُم مِّنْ أَنفُسِكُمْ أَزْوَاجًا وَجَعَلَ لَكُم مِّنْ أَزْوَاجِكُم بَنِينَ وَحَفَدَةً وَرَزَقَكُم مِّنَ الطَّيِّبَاتِ Allah adakulengerani akazi …
Read More »Ma Sunnah Komanso Miyambo Yokaonera Odwala 2
4. Mukamayendera odwala, pemphani dua iyi: لا بَأْسَ طَهُورٌ إِنْ شَاءَ اللهُ Palibe chifukwa chodera nkhawa, insha-Allah kudzera mu matendawa, muyeretsedwa. Mukhozanso kubwereza dua iyi kasanu ndi kawiri: أَسْأَلُ اللهَ الْعَظِيمَ رَبَّ الْعَرْشِ الْعَظِيمِ أَنْ يُشْفِيكَ Ndikumupempha Allah Wamphamvu zoposa, Mbuye wa Mpando Wachifumu waukulu, kuti akuchizeni. عن ابن عباس …
Read More »Sayyiduna ‘Abdur Rahmaan bin ‘Auf (Radhiyallahu ‘anhu) apatsidwa Udindo osankha Khalifah.
Pambuyo pake, Sayyiduna “Umar (radhiyallahu ‘anhu) adapanga Shura (gulu la akuluakulu omwe azipanga ziganizo) lokhala ndi ma Swahaabah asanu ndi mmodzi otsatirawa: Ali (radhiyallahu ‘anhu), ‘Uthmaan (radhiyallahu ‘anhu), Zubair (radhiyah ‘anhu) Sa’d (Radhiyallahu ‘anhu) ndi Abdur Rahmaan bun ‘Auf (radhiyallahu ‘anhu). Pankhani ya ma Sahaabah asanu ndi mmodziwa (Radhiyallahu ‘anhum), …
Read More »Ma Sunnah Komanso Miyambo Yokaonera Odwala
1. Ndi mustahab (zofunika kwambiri) kupanga wudhu usanakamuyendere odwala.[1] Olemekezeka Anas Radhwiyallahu anhu akusimba kuti Rasulullah swallallahu alaihi wasallam adati; “Amene wapanga wudhu wangwiro (pokwaniritsa masunnah ndi ma mustahab onse a wudhu) ndi kupita kukacheza ndi m’bale wake wachisilamu yemwe akudwala ndi chiyembekezo cholandira malipiro oyendera odwala, munthu oteroyo adzaikidwa …
Read More »Kuopa kwa Olemekezeka Abdur Rahman bin Auf (radhiyallahu ‘anhu) kufunsidwa
Naufal bin lyaas al Huzali (rahimahullah) adati: ‘Tikakhala pamodzi ndi Abdur Rahman bin Auf (Radhwiyallahu ‘anhu), ndi kukhala naye chifupi kodabwitsa kusangalatsirenji. Tsiku lina, anatitengera kunyumba kwake kuti tikadye, Titakhala pansi kuti tidye ndipo mbale ya chakudya ya nyama ndi mkate inaperekedwa pamaso pathu, iye adayamba kulira. Tidamufunsa: “Nchiyani chikukupangitsa …
Read More »Maonekedwe a chithupithupi cha Dajjaal
M’mahadithi olemekezeka, Olekezeka Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) adatsimikizira ummah za Maonekedwe a Dajjaal a umunthu. Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) kufotokoza za Dajjaal m’maonekedwe a munthu zikuonetsa kuti Dajjaal ndi munthu. Pa chifukwa chimenechi, chikhulupiriro cha Ahlus Sunnah wal Jamaa’ah ndi chakuti Dajjaal ndi munthu, ndipo adzabwera pa dziko lapansi nthawi …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu