Chilungamo Cha Sheikh Abdul Qadir Jeelani (rahimahullah)

Sheikh Abdul Qaadir Jeelani (rahimahullah) anali Aalim ndi Wali wa Allah Ta‘ala yemwe anakhalapo m’zaka za mma 600 A.H. Allah Ta‘ala adamudalitsa ndi kulandiridwa kwakukulu kotero kuti anthu ambiri adasintha miyoyo yawo ndi iye. Khalidwe limodzi lodziwika bwino lomwe lidawonekera m’moyo wake linali chilungamo (kuyankhula chilungamo). Pansipa pali nkhani yomwe …

Read More »

Kulowa Chisilamu kwa Abu Zar (radhwiyallahu ‘anhu)

Khalidwe lake Asanalowe Chisilamu: Asanalowe Chisilamu, Abu Zar (radhwiyallahu ‘anhu) anali chigawenga. Anali olimba mtima kwambiri kotero kuti popanda kuthandizidwa ndi anzake ena, ankakwanitsa yekha kubera anthu ndikuwachita uchifwamba. Nthawi zina, ankaukira anthu apaulendo atakwera pahatchi, ndipo nthawi zina, ankaukira akuyenda pansi. (Siyar A’laam min Nubalaa 3/373) Pambuyo pake, anasiya …

Read More »

Bilaal (Radhwiyallahu ‘anhu) Kubwerera ku Madina Munawwarah

́Allaamah Zurqaani (Rahimahullah) wapereka nkhani iyi kuchokera kwa Haafiz ibn ‘Asaakir (rahimahullah) ndi mndandanda wamphamvu wa osimba nkhani: Atamwalira Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam), zinali zovuta kwa olemekezeka Bilaal (radhwiyallahu ‘anhu) kupitiriza kukhala ku Madinah Munawwarah cha okondeka wake kwambiri Rasulullah (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam) ndi …

Read More »

Ubwino wa Jumuah

Kukhululukidwa Kwa Machimo kudzera mukuswali Jumuah Abu Hurairah (radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (swallallahu alaihi wasallam) adati: “Machimo omwe achitika pakati pa Jumu’ah ziwiri, ngati sali machimo akuluakulu, Allah amakhululuka. Tsiku Lopatulika kwa Okhulupirira Ibnu Abbaas (radhwiyallahu anhuma) adanena kuti Mtumiki (swallallahu alaihi wasallam) adati: “Tsiku ili (tsiku la Jumu’ah) …

Read More »

Dua ya Bilaal (Radhwiyallahu ‘anhu) kuwapemphera chiongoko ma Quraish.

Olemekezeka ‘Urwah bun Zubair (rahimahullah) anasimba kuti mkazi wina wa m’banja la Banu Najjaar (yemwe ndi Nawwaar bint Maalik, mayi ake a Zaid bin Thaabit (radhwiyallahu ‘anhuma)) adati: “Nyumba yanga inali pamalo okwera ndipo inali imodzi mwa nyumba zapamwamba za Mus. “Bilaal (Radhwiya Allaahu ‘anhu) ankaitana azaan ya Fajr kuchokera …

Read More »

Jumuah

Tsiku la Jumu’ah ndi lofunikira kwambiri mu Chisilamu. Izi ndi zina mwa zabwino zazikulu za Allah pa Ummah uwu ndipo ndichinthu chodziwika bwino m’Chisilamu. Rasulullah (sallallahu ‘alaihi wasallam) adati: “Tsiku la Jumu’ah ndi sayyidul ayyaam (lomwe ndi mtsogoleri wa masiku onse), ndi tsiku lalikulu kwambiri (kuchokera m’masiku a msabata) pamaso …

Read More »

Olemekezeka Bilaal (Radhwiya Allaahu ‘anhu) Ayang’anira ndi Kusunga Mkondo wa Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wa sallam)

Mfumu yaku Abysinia (Najaashi (rahimahullah)) nthawi ina inatumiza mikondo itatu kwa Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wa sallam) ngati mphatso. Atalandira mikondo itatu ija, Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wa sallam) adapereka mkondo umodzi kwa Ali (radhwiyallahu ‘anhu), adapereka mkondo wachiwiri kwa Umar (Radhwiyallahu ‘anhu) ndipo adadzisungira yekha …

Read More »

Kumasuridwa kwa Hazrat Bilaal (Radhwiya Allaahu ‘anhu) ndi Nabiy (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam) kufuna kuti Hazrat Bilaal (Radhwiyallahu ‘anhu) amasuridwe.

Nthawi ina pamene ankalankhula za Hazrat Bilaal (Radhiyallahu ‘anhu), Hazrat Sa’eed bun Musayyib (rahimahullah) adati: khumbo lofuna kulowa Chisilamu linali lalikulu kwambiri mu mtima mwa Hazrat Bilaal (radhwiyallahu ‘anhu). Adakumana ndi mavuto ndi mazunzo osalekeza kuchokera kwa anthu osakhulupirira. Nthawi zonse anthu osakhulupirira akafuna kumukakamiza kusiya Chisilamu, iye adali kukana …

Read More »

Tafseer Ya Surah Naazi’aat

وَالنَّازِعَاتِ غَرْقًا ‎﴿١﴾‏ وَالنَّاشِطَاتِ نَشْطًا ‎﴿٢﴾‏ وَالسَّابِحَاتِ سَبْحًا ‎﴿٣﴾‏ فَالسَّابِقَاتِ سَبْقًا ‎﴿٤﴾‏ فَالْمُدَبِّرَاتِ أَمْرًا ‎﴿٥﴾ Ndikulumbirira (angelo) amene amachotsa (mizimu ya osakhulupirira) mwaukali, ndi (angelo) amene amachotsa (miyoyo ya okhulupirira) moleza, ndi (Angelo) amene amasambira nayo mizimuyo (m’mlengalenga), ndi (Angelo) amene amapikisana (kukwaniritsa malamulo a Allah Ta’ala). Monga ziliri kuti Sura Nabai idavumbulutsidwa kuti idzakhazikitse chikhulupiriro cha tsiku la …

Read More »

Sunnats Ndi Aadaab Za Salaam 10

30. Popanga musaafah, ingogwirani manja a munthuyo, Palibe chifukwa chogwirana chanza ndikumavinitsa monga amachitira ma kuffaar. Chimodzimodzinso sizoyenera kupanga musaafahah uku ndikumapsopsona dzanja lake ndikumasisita pachifuwa chake popeza machitidwewa alibe maziko mu Dini. 31. Popanga musaafah, musagwire manja a munthu winayo momufinya mpaka kumupweteka. 32. Musafulumire kuchotsa manja anu mukapanga …

Read More »