Mariziq Ali M’manja Mwa Allah Yekha

Cholengedwa chilichonse chimafunikira kudya kuti chipitilire kukhala ndi moyo, ndipo chakudya chili m’manja mwa Allah yekha. Ziyenerezo, mphamvu ndi luntha sizizindikiro zodziwira umoyo wa munthu. Mawu a ndakatulo ndi oonadi: ينال الفتى من عيشه وهو جاهل ويكدى الفتى في دهره وهو عالم ولو كانت الأرزاق تجرى على الحجى هلكن إذا …

Read More »

Ubwino Owerenga Quraan Majeed 3

Ntchito Yokondedwa Kwambiri Kwa Allah ndi Kuwerenga Qur’an mosalekeza Ibnu Abbaas (radhwiyallahu anhuma) akusimba kuti munthu wina adamufunsa Rasulullah swallallahu alaihi wasallam kuti, “Kodi ndi ntchito iti yomwe ili yokondedwa kwambiri kwa Allah? Mtumiki (swallallahu alaihi wasallam) anayankha kuti, ‘Ntchito za halaal ndi murtahil (wapaulendo amene akaima paulendo wake, amayambiranso …

Read More »

Sayyiduna Ali (Radhwiyallaahu ‘anhu) kutumidwa ndi Mtumiki (Swallallaahu ‘alayhi wasallam) kuti akakonze mitumbira ya Manda, kuswa Mafano ndi kufuta Zithunzi

Olemekezeka Ali (radhwiyallahu ‘anhu) akusimba kuti nthawi ina, Mtumiki (swallallaahu ‘alayhi wasallam) adapita ku maliro a Swahaabah wina wake. Kenako adalankhula ndi ma swahaabah (radhiyallahu ‘anhum) omwe adalipo Ndipo adati: “Ndani mwa inu adzabwerera ku Madinah Munawwarah, ndipo paliponse akakawona fano kapena chiboliboli adzaziphwanya, ndipo paliponse pamene akaone mtumbira wa …

Read More »

Allah Ta’ala Yekha Ndi Amene Amadyetsa Zolengedwa Zonse

Tsiku lina, m’nthawi ya Mtumiki (swallallahu alaihi wasallam) gulu la maswahaaba a fuko la Banu Al-Ash’ar lidayenda kuchokera ku Yemen kupita ku Madina Munawwarah ndi cholinga chopanga hijrah. Atafika ku mzinda odalitsika wa Madinah Munawwarah, adapeza kuti chakudya chawo chomwe adabwera nacho chatha. Choncho adaganiza zotumiza mmodzi mwa maswahaba awo …

Read More »

Tafseer Ya Surah Faatihah

بِسْمِ اللَّهِ الرَّحْمَٰنِ الرَّحِيمِ ‎﴿١﴾‏ الْحَمْدُ لِلَّهِ رَبِّ الْعَالَمِينَ ‎﴿٢﴾‏ الرَّحْمَٰنِ الرَّحِيمِ ‎﴿٣﴾‏ مَالِكِ يَوْمِ الدِّينِ ‎﴿٤﴾‏ إِيَّاكَ نَعْبُدُ وَإِيَّاكَ نَسْتَعِينُ ‎﴿٥﴾‏ اهْدِنَا الصِّرَاطَ الْمُسْتَقِيمَ ‎﴿٦﴾‏ صِرَاطَ الَّذِينَ أَنْعَمْتَ عَلَيْهِمْ غَيْرِ الْمَغْضُوبِ عَلَيْهِمْ وَلَا الضَّالِّينَ ‎﴿٧﴾‏ Kuyamikidwa konse ndi kwa Allah, Mbuye wa zolengedwa zonse. Wachifundo Chambiri, Wachisoni. Mbuye wa tsiku lachiweruzo. Inu nokha timakupembedzanindipo kwa Inu nokha ndi kumene timakupemphani chithandizo. Tiwonetseni …

Read More »

Mtsutso Wa Pakati Pa Nabi Ebrahim (alaihis salaam) Ndi Namruud

Namrud idali mfumu yopondereza komanso yankhanza imene inkanena kuti iye ndi mulungu ndipo inkalamula anthu kuti adzimulambira. Nabi Ebrahim (alaihis salaam) atapita kwa Namrud ndikumuitanira ku umodzi wa Allah, Namrud chifukwa cha kudzikweza kwake ndi kukakamira kwake, sadavomere ndipo adafunsa Nabi Ebrahim (alaihis salaam) kuti angachite chiyani Mbuye wake. Nabi …

Read More »

Ubwino Owerenga Quraan Majeed 2

Mngelo Kuteteza Mphotho Sayyiduna Ali (radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (swallallahu alaihi wasallam) adati: “Munthu akagwiritsa ntchito miswaak kenako n’kuimirira kuswali, mngelo amaima pambuyo pake ndikumvetsera kuwerenga kwake Qur’an Majiid. Kenako mngeloyo amayandikira kwa iye mpaka kukumanitsa pakamwa pake ndi pakamwa pake (pa owerengayo). gawo lilichonse la Qur’an Majiid lomwe …

Read More »

Chilungamo cha Ali (radhwiyallahu ‘anhu)

Ali bun Rabii’ah akusimba kuti nthawi ina Ja’dah bin Hubairah (radhwiyallahu ‘anhu) adadza kwa Ali (radhwiyallahu ‘anhu) nati: “E inu Amiir-ul-Mu’miniin! Anthu awiri akabwera kwa inu (ndi mkangano wawo) Mmodzi mwa awiriwo amakukondani kwambiri kuposa banja lake ndi chuma chake, pomwe winayo ndi woti akadakhoza kukuphani, akadachita. choncho (chifukwa cha …

Read More »

Ubwino Owerenga Quraan Majeed

Muuni Padziko Lapansi ndi chuma cha tsiku lachiweluzo Abu Zarr (radhwiyallahu anhu) anati: “Nthawi ina ndinamufunsa Mtumiki (swallallahu alaihi wasallam) kuti, ‘E, Mtumiki (swallallahu alaihi wasallam), chonde ndipatseni malangizo.” Mtumiki (swallallahu alaihi wasallam) anayankha: “Igwiritsitse taqwa; Adati: “E, Mtumiki (swallallahu alaihi wasallam), chonde ndipatseninso malangizo ena.” Mtumiki (swallallahu alaihi wasallam) …

Read More »