Naufal bin lyaas al Huzali (rahimahullah) adati: ‘Tikakhala pamodzi ndi Abdur Rahman bin Auf (Radhwiyallahu ‘anhu), ndi kukhala naye chifupi kodabwitsa kusangalatsirenji. Tsiku lina, anatitengera kunyumba kwake kuti tikadye, Titakhala pansi kuti tidye ndipo mbale ya chakudya ya nyama ndi mkate inaperekedwa pamaso pathu, iye adayamba kulira. Tidamufunsa: “Nchiyani chikukupangitsa …
Read More »Maonekedwe a chithupithupi cha Dajjaal
M’mahadithi olemekezeka, Olekezeka Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) adatsimikizira ummah za Maonekedwe a Dajjaal a umunthu. Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) kufotokoza za Dajjaal m’maonekedwe a munthu zikuonetsa kuti Dajjaal ndi munthu. Pa chifukwa chimenechi, chikhulupiriro cha Ahlus Sunnah wal Jamaa’ah ndi chakuti Dajjaal ndi munthu, ndipo adzabwera pa dziko lapansi nthawi …
Read More »Kulandira Uthenga Wabwino Wamwayi Ndi Chikhululukiro M’maloto
Usiku wina, Hazrat Abdur Rahmaan bin Auf (Radhwiyallahu ‘anhu) adakomoka kwa nthawi yayitali chifukwa chakudwala kwake mpaka omwe anali pafupi naye adaganiza kuti mzimu wake wachoka. Anamuphimba ndi nsalu n’kuchokapo. Mkazi wake, Ummu Kulthum bint ‘Uqbah, nthawi yomweyo adapempha thandizo kwa Allah Ta’ala podekha ndi kuswali (monga talamulidwa kutero mu …
Read More »Abdur Rahmaan bin Auf (Radhwiyallahu ‘anhu) agwiritsa ntchito Chuma chake pa nkhondo ya Tabuk.
Pamene Allah Ta’ala ankamulamula Rasulullah (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) kuti anyamuke ulendo wa ku Tabuk, ma Swahaabah ambiri adalibe kalikonse panthawiyo zoti athandizikirw kuyende ulendo wautali ndi wotopetsa, makamaka pamene ankayembekezera kukumana ndi gulu lankhondo lachiroma pankhondo yomwe inali ndi zida zokwanira komanso adalipo ambiri. Choncho pofuna kusonkhanitsa pamodzi ndi …
Read More »Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wa sallam) Kusankha Abdur Rahmaan bin Auf (radhwiya Allahu ‘anhu) kukhala Mtsogoleri wa Asilikali pa nkhondo ya Dumatul Jandal.
M’chaka cha chisanu ndi chimodzi chioangireni Hijrah, m’mwezi wa Sha’baan, Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam) adalankhula ndi Abdur Rahmaan bin Auf (Radhwiyallahu ‘anhu) nati kwa iye: “Konzekeretsa ulendo wako, popeza ndikufuna ndikutumize ku ulendo, mwina lero kapena mawa, Insha Allah. M’mawa mwake, Abdur Rahmaan bun Auf (Radhiyallahu ‘anhu) …
Read More »Mantha a Abdur Rahman bin Auf (Radhwiyallahu ‘anhu) kuyankha mlandu ngakhale adawonongera chuma pa ntchito ya Dini.
Shu’bah (Rahimahullah) akuti: Nthawi ina Abdur Rahman bun Auf (Radhwiyallahu ‘anhu) ankasala kudya ndipo nthawi ya iftaar, chakudya chinabweretsedwa kwa iye. Ataona chakudyacho, Abdur Rahman bin Auf (Radhwiyallahu ‘anhu) adati: “Hamzah (Radhwiyallahu ‘anhu) adaphedwa chifukwa cha chikhulupiriro ndipo sitinapeze nsalu yokwanira sanda yake, ndipo anali wabwino kuposa ine. Mus’ab bin …
Read More »Kuwolowa manja kwa Abdur Rahmaan bin Auf (Radhiyallahu ‘anhu)
Miswar bin Makhramah (Radhwiyallahuanhu) akuti: Abdur Rahmaan bun Auf (Radhwiyallahu ‘anhu) nthawi ina adagulitsa munda wa mpesa kwa Uthman (Radhwiyallahu ‘anhu) pamtengo wa ma dinari zikwi makumi anayi (40,000). Abdur Rahmaan (Radhwiya Allaahu ‘anhu) atalandira ndalamazo kuchokera kwa Uthmaan (Radhwiyallahu ‘anhu), nthawi yomweyo adazigawa kwa akazi odalitsika a Mtumiki (Swalla …
Read More »Abdur-Rahman bin Awf (Radhwiyallahu ‘anhu) amatsogolera Swalaah
Paulendo wa Tabuuk, ma Swahaabah (Radhwiyallahu ‘anhum) adali pa ulendo ndi Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam). Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) adachoka kwa ma Swahaabah (Radhwiyallahu ‘anhum) kuti apite kukazithandiza. Popeza kuti nthawi ya Swalah ya Fajr sidali yochuluka, ndipo ma Swahaabah (Radhwiyallahu ‘anhum) ankaopa kuti nthawi itha kutha, sadamudikire …
Read More »Zizindkiro za Qiyaamah 5
Chikhulupiriro cha Ahlus Sunnah wal Jamaa’ah pa nkhani ya Dajjaal Kutulukira komanso kubwera kwa ma fitnah a Dajjaal zimayendera limodzi m’zitaab za Aqaa’id (Zikhulupiriro za Chisilamu). Ma Ulama a Aqaa’id amavomereza kuti kukhulupirira kutulukira kwa Dajjaal ndi gawo la Aqaa’id ya Ahlus Sunnah wal Jamaa’ah. Mahadith omwe mkati mwake Mtumiki …
Read More »Ubwino Oyendera Odwala 2
Kutalikitsidwa ndi Jahannam kwa ntunda okwana kuyenda zaka makumi asanu ndi awiri (70) Olemekezeka Anas (Radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) adati: “Amene wapanga wudhu olongosoka (pokwaniritsa masunnah ndi ma mustahabbaat) ndi kupita kukamuona m’silamu nzake yemwe akudwala ndi chiyembekezo choti adzalandire malipiro okayendera nsilamu odwala, munthu oteroyo …
Read More »