Dua ya Mtumiki (swallallaahu ‘alayhi wasallam) kwa Ali (radhwiyallahu ‘anhu) potumiza ku Yemen

Ali (radhwiyallahu ‘anhu) akuti: Rasulullah (swallallaahu ‘alayhi wasallam) adanditumiza monga bwanamkubwa wake ku Yemen. Ndisananyamuke ndidalankhula naye ndipo ndidati: “E, Mtumiki (swallallaahu ‘alayhi wasallam)! Inu mukunditumiza kwa anthu akuluakulu kuposa ine. Kuonjezera apo, ine ndiine mwana, ndipo ndilibe kuzindikira kulikonse pa kaweruzidwe kamilandu. Atamva nkhawa zanga, Rasulullah (swallallaahu ‘alayhi wasallam) …

Read More »

Kugula Malo Oonjezera Musjid-ul-Haraam

Nthawi ina Mtumiki (swallallaahu ‘alayhi wasallam) adapita kwa munthu wina ku Makkah Mukarramah ndipo anati kwa iye, “O wakuti-ndi-wakuti! Kodi ungandigulitseko nyumba yako, kuti ndiwonjezereko nzikiti mozungulira Ka’bah, ndipo mu mphotho ya ntchito yabwinoyi, ndikukutsimikizira kuti udzakhala ndi nyumba yachifumu ku Jannah (kuwonjezera pa ndalama za nyumba yomwe utapatsidwe)?” Munthuyo …

Read More »

Qunuut

3. Ndi sunnah kuswali Swalah ya Witr tsiku lililonse m’chaka chonse. Swalah ya Witri idzachitika mukatsiriza kuswali Fardh ndi Sunnah za Swalah ya Esha. M’chaka chonse, munthu akaswali Witr sangawerenge Qurnuot. Komabe zili sunnah kuwerenga Ounoot mu pa swala ya Witr mu theka lachiwiri la mwezi wa Ramadhaan (kuyambira pa …

Read More »

Kukonzekera nkhondo ya Tabuuk

Abdur Rahmaan bun Khabbaab (radhwiyallah anhu) akufotokoza motere: Ndinalipo pamene Mtumiki (swallallaahu ‘alayhi wasallam) ankawalimbikitsa ma Swahaabah (radhwiyallahu ‘anhum) kuti akonzekeretse asilikali ndi kutenga nawo gawo pa ulendo wa Tabuuk. Nthawi imeneyo Uthmaan (radhwiya allahu ‘anhu) adayimilira nati: “Oh Mthenga wa Allah (swallallaahu ‘alayhi wasallam)! Ine ndikupereka ngamila zana limodzi …

Read More »

Qunuut

1. Ndi Sunnah kuwerenga Qunuut mu rakah yachiwiri ya Swalah ya Fajr. Qunuut idzawerengedwa mu rakah yachiwiri akaweramuka kuchokera pa Ruku. Adzayambe wawerenga tahmeed (ربنا لك الحمد) kenako adzayamba kuwerenga Qunut. 2. Powerenga Qur’an, munthu adzakweza manja ake mpaka pa chifuwa chake ndikuwerengaa dua monga momwe munthu amanyamulira manja ake …

Read More »

Kukhudzika pa Nkhani ya Kuyankha Mafunso pa Tsiku Lomaliza

Nthawi ina yake “Uthmaan (radhwiyallahu ‘anhu) adalowa m’khola lake la ziweto ndipo adapeza kapolo wake akudyetsera ngamira. Atachiona chakudyacho Uthmaan (radhwiyallahu ‘anhu) sadasangalatsidwe ndi mmene kapoloyo adachikonzera  kotero adapotokora khutu lake. Patangopita nthawi pang’ono, atalingalira zomwe wachita, ‘Uthmaan (radhwiyallahu ‘anhu) adada nkhawa ndikuopa kuti sangamutsegulire mlandu pa zimene wachita tsiku …

Read More »

Imaam Abu Hanifah Ndi Mafunso Atatu A Mfumu Ya Chiroma

Mfumu yachiroma ulendo wina inatumiza chuma chambiri kwa Khalifa (Mtsogoleri) wa asilamu. isanatumize nthumwi yake ndi chumacho, Mfumuyi inamulamula kuti akafunseko mafunso atatu kwa ma Ulama achisilamu. Nthumwi yachiromayi monga idauzidwira, idafunsa mafunso atatu aja kwa ma Ulama koma sanathe kumupatsa mayankho okhutira. Pa nthawiyo Imaam Abu Hanifah anali mnyamata …

Read More »

Qadah ndi Salaam

7. Ngati ili qa’dah yomaliza, werengani tashahhud, Salawaat Ebrahimiyyah (Durood Ebrahim) ndipo kenako pangani duwa. Duruud Ebrahimiyyah (Durood Ebrahim) ili motere: اَللّٰهُمَّ صَلِّ عَلٰى مُحَمَّدٍ وَّعَلٰى اٰلِ مُحَمَّدٍ كَمَا صَلَّيْتَ عَلٰى إِبْرَاهِيْمَ وَعَلٰى اٰلِ إِبْرَاهِيْمَ وَبَارِكْ عَلٰى مُحَمَّدٍ وَّعَلٰى اٰلِ مُحَمَّدٍ كَمَا بَارَكْتَ عَلٰى إِبْرَاهِيْمَ وَعَلٰى اٰلِ إِبْرَاهِيْمَ فِيْ الْعَالَمِيْنَ …

Read More »

Makhalidwe khumi apadera a Uthmaan (radhwiyallahu anhu)

Hazrat Abu Thawr (rahimahullah) akuti tsiku lina adadza kwa Uthmaan (radhwiyallah”anhu) ndipo adamumva akunena izi panthawi yomwe adaukiridwa. Adati: “Pali ntchito zabwino zokwana khumi zomwe ndadziteteza kwa Allah Taala, ndipo pa ntchito iliyonse ndikuyembekeza kudzalandira malipiro pa tsiku lomaliza; 1) Ndinali munthu wachinayi kuvomereza Chisilamu. 2) Sindinanenepo bodza moyo wanga …

Read More »

Rakaah Yachiwiri

1.Pamene mukudzuka kuchoka pa sajdah, choyamba kwezani chipumi ndi mphuno, kenako zikhato kenako mawondo. 2.Pamene mukuimirira Rakaah yachiwiri, gwirani pansi poika manja anu onse pansipo kuti muthandizikire kunyamuka. 3.Pempherani rakaah yachiwiri monga mwa nthawi zonse (kupatula Dua-ul Istiftaah). Qadah ndi Salaam 1. Pambuyo pa sajda yachiwiri ya rakaah yachiwiri, khalani …

Read More »