Njira Yopezera madalitso Ndi kudzitetezera Kwa Adani Olemekezeka Jaabir bin Abdillah akusimba kuti Rasulullah (Swallallahu alaihi wasallam) adauza maSwahaabah kuti: “Kodi sindingakusonyezeni njira yoti mupulumutsidwe kwa adani anu ndi kulandira zochuluka m’zimene muli nazo? Tembenukirani kwa Allah usiku ndi usana chifukwa dua ndi chida cha okhulupirira.”[1] Mngelo Apangira Dua Munthu …
Read More »Kufunika Kwa Dua 2
Dua Kupindulira Munthu Mnthawi ino ndi Mtsogolo Olemekezeka Ibnu Umar (Radhwiyallahu anhuma) akusimba kuti Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) adati: “Dua imapindulitsa pakalipano komanso mtsogolo. Choncho, inu akapolo a Allah, pirirani popempha.[1] Yemwe amapanga Dua nthawi zonse Amapindula Olemekezeka Abu Sa’iid Khudri (Radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) adati: …
Read More »Kufunika Kwa Dua 1
Chida cha okhulupirira Olemekezeka Ali (Radhwiyallahu anhu) anasimba kuti Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) adati:“Dua ndi chida cha okhulupirira, Mzati wa Dini, ndi Nuur (kuwala) yakumwamba ndi pansi.”[1] Dua ndi gwero la Ibaadah Olemekezeka Anas (radhwiyallahui anhu) akusimba kuti Rasulullah (Swallallahu alaihi wasallam) adati:”Dua ndiye maziko a ibaadah.”[2] Allah amasangalatsidwa pamene …
Read More »Dua
Dua ndi njira yomwe kapolo amadziyandikitsira nayo ku chuma chopanda malire cha Allah. Pali zabwino zambiri zomwe zanenedwa Mmahadith kwa amene amapanga dua. Rasulullah (Swallallahu alaihi wasallam) adanena kuti dua ndiye maziko a ibaadah zonse. Mu Hadith ina, Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) adanena kuti Allah amakondwera ndi kapolo amene amapanga …
Read More »Surah Zokhala ndi nthawi zake zowerenga komanso nthawi zake zosiyanasiyana zomwe zikuyenera kuwerenga 4
9. Werenganinso ayah zitatu zomaliza za Surah Baqarah musanagone. Kwanenedwa kuti Ali (Radhwiyallahu anhu) adati: “Sindikuganiza kuti aliyense wanzeru angagone popanda kuwerenga ma aya (atatu) omaliza a Surah Baqarah, chifukwa ndithu iwowo ndi chuma chochokera pansi pa Arsh. 10. Werengani Surah Faatihah ndi Surah Ikhlaas musanagone. Anas (Radhwiyallahu anhu) akusimba …
Read More »Surah Zokhala ndi nthawi zake zowerenga komanso nthawi zake zosiyanasiyana zomwe zikuyenera kuwerenga 3
6. werengani Surah Sajdah musanagone. Olemekezeka Jaabir (Radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) sankagona mpaka atawerenga Surah Sajdah ndi Surah Mulk.[1] Khaalid bin Ma’daan rahimahullah, Taabi’ee, adatchula izi: “Ndithu Surah Sajdah idzakangana m’manda poteteza amene ankaiwerenga. Idzati, ‘O, Allah! Ngati ndili ochokera ku chitaab Chanu, muvomereni chiwombolo changa …
Read More »Surah Zokhala ndi nthawi zake zowerenga komanso nthawi zake zosiyanasiyana zomwe zikuyenera kuwerenga 2
4. Werengani Surah Yaasiin m’mawa ndi madzulo aliwonse. Ibnu Abbaas (Radhwiyallahu anhu) adati: “Amene angawerenge Surah Yaasiin m’bandakucha, ntchito yake ya tsiku lonse idzafewetsedwa, ndipo amene angaiwerenge madzulo, ntchito yake mpaka m’mawa idzafewetsedwa.”[1] Olemekezeka Jundub (Radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) anati: “Amene angawerenge Surah Yaasiin usiku ndi …
Read More »Surah Zokhala ndi nthawi zake zowerenga komanso nthawi zake zosiyanasiyana zomwe zikuyenera kuwerenga
Pali Surah zina zomwe zalamuridwa kuti ziziwerengedwa nthawi yodziwika usiku ndi usana kapena masiku ena a sabata. Ndi mustahab kwa munthu kuwerenga ma surah amenewa mu nthawi yake yoikidwa. 1. Werengani Surah Kaafiroon musanagone. Olemekezeka Jabalah bun Haarithah (Radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (Swallallah alaihi wasallam) adati: “Ukamakagona, werenga Surah …
Read More »Sunnah komanso miyambo yoyenera kutsatira usanayambe Kuwerenga Quraan Majiid 10
23. Ngati mudaloweza pamtima gawo lina lake la Qur’an Majiid, onetsetsani kuti mukulibwereza nthawi zonse kuti musaiwale. Hadith yachenjeza za kunyalanyaza kuwerenga Quraan ndi kuiwala zomwe waloweza pamtima.[1] Olemekezeka Abu Musah Ash’ari (radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Rasulullah Adati: “Isamareni Qur’an Majiid. Ndikulumbirira Amene m’manja Mwake muli moyo wanga, (Qur’an Majiid) …
Read More »Sunnah komanso miyambo yoyenera kutsatira usanayambe Kuwerenga Quraan Majiid 9
21. Mukamaliza kuwerenga Qur’an yonse mpaka kukafika Surah Naas, zili mustahab kuti muyambirenso kuwerenga poyambiranso ndi Surah Faatihah ndi aya zoyambira za Surah Baqarah mpaka ulaaika humul muflihuun. 22. Mukamaliza kuwerenga Quraan yonse, werengani dua iyi: اَللّٰهُمَّ ارْحَمْنِيْ بِالْقُرْآنْ وَاجْعَلْهُ لِيْ إِمَاماً وَّهُدًى وَّرَحْمَةً اَللّٰهُمَّ ذَكِّرْنِيْ مِنْهُ مَا نَسِيْتُ وَعَلِّمْنِيْ …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu