1 Mizikiti imatengedwa kuti ndimalo okondedwa kwambiri pamaso pa Allah. عن أبي هريرة رضي الله عنه أن رسول الله صلى الله عليه وسلم قال أحب البلاد إلى الله مساجدها وأبغض البلاد إلى الله أسواقها (صحيح مسلم، الرقم: 671) Sayyiduna Abu Hurairah (radhiyallahu anhu) akufotokoza kuti Mtumiki (Sallallahu alaih wasallam) adati: …
Read More »Nthawi Zimene Miswak Ikufunika Kugwirtsidwa Ntchito
7. Pamene wina ali kumapeto kwa moyo wake (ali pafupi kumwalira).
Sayyidatuna Aisha (radhiyallahu anha) akufotokoza kuti, Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) atatsala pang’ono kumwalira nchimwene wanga amene ndi AbdulRahmaan (radhiyallahu anhu) adalowa mchipinda chomwe Mtumiki (sallallah alaih wasallam) adagona atanyamula miswaak yomwe ankagwiritsa ntchito kutsukira mkamwa.
Read More »Nthawi Zimene Miswak Ikufunika Kugwirtsidwa Ntchito
4. Pamene mukupanga wuzu.
Sayyiduna Abu Hurairah (radhiyallahu anhu) akuakufotokoza kuti Mtumiki (sallallahu alaih Wasalaam) adati, “chikhala kuti sichipsinjo pa ummah wanga ndikadawalamula (ndikadazipanga kukhala zokakamiza) kuti adzigwiritsa ntchito miswaak nthawi inailiyonse pamene akupanga wudhu (komano Sizili zokakamiza kutero koma ndisunnah yomwe yalimbikitsidwa pamene mukupanga wudhu).”
Read More »Nthawi Zimene Miswak Ikufunika Kugwirtsidwa Ntchito
1. Mukangodzuka kumene.
Sayyiduna Aishah radhiyallahu anha akusimba kuti, nthawi zonse Mtumikisallallahu alaih wasallam ankati akadzuka, kaya ndimasana kapena usiku ankatsuka mkamwa ndi miswak asanapange wudhu.’’
Read More »Njira Ya Sunnah Yogwiritsira Ntchito Miswaak (mswachi ochokera ku mtengo)
4. Mukatsiriza kugwiritsa ntchito miswaak, utsukeni ndipo uyikeni choimika.[1] 5. Ngati palibe Miswaak, Chala sichingalowe m’malo mwa miswak, Kotero munthu adzayenera kugwiritsa ntchito chinthu chokhuthala chimene chingathe kuyeretsa mkamwa, monga nswachi (toothbrush).[2] 6. Miswaak siwoyenera kuti utali wake upambane chikhatho chadzanja limodzi.[3] 7. Kamtengo kali konse komwe kamakhala bwino kuchukuchira …
Read More »Njira Ya Sunnah Yogwiritsira Ntchito Miswaak (mswachi ochokera ku mtengo)
1. Njira yogwilira miswaak ili motere, Munthu ayenere ayike chala chachikulu ndi chaching´ono pansi pa miswaak ndipo zala zake zotsalazo ayike mbali yapamwamba pa Miswaak.[1] 2. Gwirani Miswaak ndi mkono wamanja ndipo yambani kutsuka mano kuyambira mbali yakumanja.[2] 3. Tsukani mano mopingasa ndipo lilime mulitsuke molitsatira (mulitali make), chimodzimodzinso, tsukani …
Read More »Ubwino ogwiritsa ntchito miswak
1. Kugwiritsa ntchito miswak kumaonjezera sawaabu za swalah ka 70.
Sayyiduna Aaishah radhiyallahu anha akunena kuti Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) adati, swalah imene yapempheledwa utagwiritsa ntchito miswak (popanga wudhu) ilindi sawaab zokwana 70 kuposa swalah yomwe yaswalidwa popanda kugwiritsa ntchito miswak.
Read More »Nthawi Zomwe Ndi Sunnah Kusambanthawi Zomwe Ndi Sunnah Kusamba
Pali nthawi zambiri zimene kusamba ndisunnah, zina mwa nthawizi ndi izi:
1.Tsiku la Jumua (lachisanu).
Sayyiduna Abullah bin Umar (radhwiyallahu anhuma) akunena kuti Mtumiki (Sallallahu alaih Wasallam) anati,” pamene wina mwainu akubwera ku swala ya Jumua (lachisanu) ayenera kusamba.”
Read More »Kasambidwe Ka Sunnah Gawo 5
Zokakamiza Posamba
Pali zinthu ziwiri zomwe ndizokakamizidwa kuchita ukamasamba,
1. Kupanga niya yosamba musanayambe kusambitsa thupi lanu.
2. Kuthira madzi thupi lonse.
Read More »Kasambidwe Ka Sunnah-Gawo 4
14. Onetsetsani kuti madzi akufika pena paliponse pathupi lanu, nthawi ina iliyonse mukadzithira madzi dzinyureni ndicholinga chofuna kuonetsetsa kuti madziwo alowa pakhungu lonse, ngakhale kutangotsala malo ochepetsetsa kwambiri osathiridwa madzi, kusamba (kwa fardh) sikudzatheka, pamene mukusambitsa thupi, sambitsani kutsogolo kwake kenako kumbuyo.
Read More »