Sahaabah

Chikondi cha olemekezeka Ali radhwiyallahu anhu pa Mtumiki Muhammad (swallallahu alaih wasallam)

Usiku umene Mtumiki (swallallahu alaih wasallam) ankasamuka kupita ku Madinah Munawwarah makafiri adazungulira nyumba yake ndicholinga choti amuphe. Mtumiki (swallallahu alaih wasallam) asadasamuke adamuuza Ali (radhwiyallahu anhu) kuti akagone ku nyumba ya Mtumiki (swallallahu alaih wasallam) ndicholinga choti makafiri aganize ngati Mtumiki (swallallahu alaih wasallam) adakali m’nyumba momwemo sadatuluke ndipo …

Read More »

Chikondi cha Hazrat Uthmaan (radhiyallahu anhu) pa Hazrat Rasulullah (sallallahu alaih wasallam)

  Nthawi ya Hudaybiyah, Hazrat Uthmaan (radhiyallahu ‘anhu) adatumidwa ndi Rasulullah (sallallahu alaih wasallam) kukakambirana ndi ma Quraish ku Makka Mukarramah. Pamene Hazrat Uthmaan (radhiyallahu ‘anhu) adanyamuka kupita ku Makka Mukarramah, ena mwa maswahabah adamchitira kaduka Uthmaan (radhiyallahu anhu) chifukwa chokwanitsa kuchita tawaaf ya nyumba ya Allah (ka’bah). Komano mthenga …

Read More »

Chikondi chakuya  komanso chikumbutso cha Umar (radhwiyallahu anhu pa Mtumiki (swallallahu alaih wasallam)

Usiku wina olemekezeka Umar (radhwiyallahu anhu) mu ulamuliro wake ali mkati moyendayenda kupereka chitetezo adaona kuwala kuchokera nyumba inayake komanso adamva mawu. Atapita komweko adapeza mayi wachikulire akuluka uku akulakatula ndakatulo iyi, عَلَى مُحَمَّدٍ صَلَاةُ الْأَبْرَارْ ** صَلَّى عَلَيْكَ الْمُصْطَفَوْنَ الْأَخْيَارْ Ndikuppha anthu onse olungama kuti apitirize kumfunira zabwino Mtumiki …

Read More »