10. Mukangoyamba Swalaah, werengani Dua-ul Istiftaah chamuntima: وَجَّهْتُ وَجْهِيَ لِلَّذِيْ فَطَرَ السَّمَاوَاتِ وَالْأَرْضَ حَنِيْفًا مُسْلِمًا وَمَا أَنَا مِنَ الْمُشْرِكِيْنَ إِنَّ صَلَاتِيْ وَنُسُكِيْ وَمَحْيَايَ وَمَمَاتِيْ لله ِرَبِّ الْعَالِمِيْنَ لَا شَرِيْكَ لَهُ وَبِذلِكَ أُمِرْتُ وَأَنَا مِنَ الْمُسْلِمِيْنَ Ndatembenukira nkhope yanga kwa Yemwe adalenga thambo ndi nthaka, ndikukhalabe panjira yoongoka popanda kusokonekera, ndikugonjera …
Read More »Kugula Chitsime ku Jannah
Pamene Masahaabah (radhiyallahu ‘anhum) adasamukira ku Madinah Munawwarah, madzi omwe adawapeza kumeneko adali ovuta kwa iwo kumwa popeza adali anchere. Komabe, padali Myuda wina yemwe amakhala ku Madinah Munawaarah yemwe adali ndi chitsime chamadzi okoma otchedwa Ruumah, ndipo ankagulitsa madzi a pachitsime chakewo kwa maswahaabah (radhiyallahu ‘anhum). Mtumiki (swallallaahu ‘alayhi …
Read More »Qiyaam
1. Yang’anani kuchibula. 2. Sungani mapazi pamodzi kapena pafupi momwe mungakwanitsire. Onetsetsani kuti mapazi ayang’ana kuchibla. 3. Pambuyo pake, pangani Niya ya Swalah yomwe mukuswali ndipo kwezani manja anu mpaka zala zanu zazikulu zigwirizane ndi nsonga zamakutu ndipo nsonga za zala zanu zikhale molingana ndi kumtunda kwa makutu anu. 4. …
Read More »Sayyiduna Umar (Radhiyallahu ‘anhu) Kulamula Zabwino Panthawi Yotsiriza (yamoyo wake)
M’mawa wa tsiku limene Sayyiduna Umar (Radhwiya Allahu ‘anhu) adabayidwa, mnyamata wina adamuyendera nati kwa iye: “Ameer-ul-Mu’mineen! Sangalalani ndi nkhani yabwino yochokera kwa Allah Ta’alal, Inu ndinu Sahaabi wa Mtumiki (Swallallaahu ‘alayhi wasallam) Ndipo inu muli m’gulu la anthu amene adalandira Chisilamu m’masiku oyambirira, ndipo mudasankhidwa kukhala Khalifa ndipo mudachita …
Read More »Tafseer ya Surah Ikhlaas
بِسْمِ اللَّهِ الرَّحْمَٰنِ الرَّحِيمِ قُلْ هُوَ اللَّهُ أَحَدٌ ﴿١﴾ اللَّهُ الصَّمَدُ ﴿٢﴾ لَمْ يَلِدْ وَلَمْ يُولَدْ ﴿٣﴾ وَلَمْ يَكُن لَّهُ كُفُوًا أَحَدٌ ﴿٤﴾ Sura iyi ikufotokoza za chikhulupiriro cha Tawhiyd (umodzi wa Allah Ta’ala mu kakharidwe kake ndi mbiri zake), zomwe ndi gawo limodzi lofunikira kwambiri m’zikhulupiliro zazikulu za Chisilamu. Chikhulupiriro cha Tawheed chinali chinthu chachilendo kwa …
Read More »Swalaah Isanayambe
1. Chisamaliro chapadera chiyenera kutengedwa povala moyenera pa Swalaah. Mkazi ayenera kuvala chovala choterocho chomwe chidzabisa thupi lake lonse ndi tsitsi lake. Ndikusadzipatsa ulemu iye mwini kuvala zovala zothina zomwe zimasonyeza mmene thupi lake lilili kapena kuvala zovala zopyapyala zimene zingachititse kuti ziwalo zenizeni ziwonekere. Ngati chovalacho chili chooneka kuti …
Read More »Hazrat Umar (radhwiyallahu anhu) Kufuna kuyikidwa pafupi ndi Rasulullah (swallallaahu alaih wasallam)
Pakati pa mphindi zomaliza pambuyo pa Hazrat Umar (radhiliyalahlah ‘Ahu) adaphedwa mwangozi, Anatumiza mwana wake, Hazrat Abdullah Bin Umar (radhwiyallahu ‘Anhuma), kunyumba kwa Hazrat Aaishah (radhiyallahu ‘ahha). Hazrat Umar (Radhiyallahu anhu adamulangiza iye kuti ukamuuze kuti Umar akupereka Salaam. Usakanene kuti Amiirul muuminiin popeza kuyambira lero sindidzaitanidwanso …
Read More »Kudzichepetsa kwa Sayyiduna Umar (Radhwiyallahu ‘anhu)
Olemekezeka Miswar bin Makhramah (radhwiyallahu ‘anhu) akusimba kuti pamene Umar (radhwiyallahu ‘anhu) anabayidwa, iye anayamba kumva chisoni ndi kukhala ndi nkhawa kwambiri kuudandaulira ummah. Ibnu Abbaas (radhwiyallahu ‘anhu) adamtonthoza nati: “Oh Ameer-ul-Mu’mineen! Palibe chifukwa chodandaulira. Mudakhala pamodzi ndi Mtumiki (swallallaahu ‘alayhi wasallam) ndipo mudakwaniritsa ma ufulu ake onse . Ubwenzi …
Read More »Mfundo Ya Imaam Shaafi’ee
Imaam Shaafi’e (rahimahullah) walemba mu chitabu chotchedwa Ikhtilaaful Hadith kuti: Sitikudziwa mwa akazi olemekezeka a Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) kusiya nyumba zawo ndikupita kunzikiti kukaswali Swalaah ya Jumuah kapena Swalah ina iliyonse, ngakhale kuti adali akazi olemekezeka a Sayyiduna Rasulullah chifukwa cha udindo wawo wapadera ndi ubale wawo ndi Mtumiki …
Read More »Ulemu wa Umar (radhwiyallahu ‘anhu) kwa Abu Bakr (radhwiyallahu ‘anhu)
Hazrat Umar (radhiyallahu anhu) nthawi zonse ankavomereza udindo wapamwamba wa Hazrat Abu Bakr (radhwiyallahu ‘anhu) ndipo sankadzitenga ngati iye ndi wofanana ndi Abu Bakr (radhwiyallahu ‘anhu). Ulendo wina gulu la anthu linamutamanda Umar (radhwiyallahu ‘anhu) ponena kuti: “Ndikulumbirira kwa Allah! Sitinaonepo munthu wolungama, wonena zoona, ndi wokhwimitsa zinthu kwambiri kwa …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu