5. Yambani ndi kuwerenga Bismillah mukamasamba, ndikupanga niya yoti mukuchotsa hadathil akbar (unve waukulu).
6. Sambitsani zikhatho zanu katatu.
Read More »5. Yambani ndi kuwerenga Bismillah mukamasamba, ndikupanga niya yoti mukuchotsa hadathil akbar (unve waukulu).
6. Sambitsani zikhatho zanu katatu.
Read More »Abu Hurairah (radhiyallahu anhu) akusimba kuti Rasulullah (sallallahu alaih wasallam) adanena kuti " nyumba zanu musazipange kukhala ngati ndi manda (zipangeni nyumba zanu kukhala za moyo popangilamo ntchito za bwino monga ngati swalah, kuwerenga Qur’aan majeed ndi zina zambiri. Choncho mukamatero nyumba zanu sizikhala ngati ndi manda kumene sikumachitikako ma aamaal abwino.) Ndipo manda anga musawatenge ngati ndi malo opangilapo zisangalalo, komanso mudziwerenga durood kwa ine, ndithudi mwa njira ina iliyonse Durood yo imandifika (kudzera mwa angelo) kuchokera kwina kuli konse komwe muli."
Read More »1. Yang’anani ku Qiblah (komwe timayang’ana tikamaswali) mukamasamba. ndibwino kuvala chovala kutchinga maliseche pamene mukusamba.
2. Sambirani malo omwe wina sangakuoneni. ndibwino kusamba mutaphimba maliseche anu. komano ngati wina ali malo omwe sangaonedwe ndimunthu wina (ngati kubafa) ngati wina akusamba maliseche, ndizoloredwa.
Read More »
Hazrat Hassan Bin Ali (radhiyallahu anhuma) akufotokoza kuti Rasulullah (sallallahu alaih wasallam) adanena kuti "Werengani durood kwa ine kwina kulikonse komwe mungakhale popeza durood yanuyo imafikitsidwa kwa ine (kudzera mwa angelo).
Read More »25. Ngati mbali iliyonse yachiwalo chomwe ndi fardh kusambitsa pamene mukupanga wudhu yasiidwa osasambitsa, wudhu udzakhala opelewera.
Sayyiduna Umar (radhwiyallahu anhu) akunena kuti munthu anapanga wudhu nasiya malo amodzi osasambitsa kuphanzi kwake mlingo wachikhadabu poyang’anitsitsa malo amenewo Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) anamuuza iye kuti “pita ukamalizitse kupanga wudhu wako.”
Read More »
Sayyiduna Abu Hurairah (radhiyallahu anhu) akufotokoza kuti, Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) adati, "amene amawerenga Qur'an, amatamanda Allah Ta'ala, amawerenga Durood kumuwerengera Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) komanso amapempha chikhululuko kwa mbuye wake ndiye kuti wapempha zabwino kuyambira pa tsinde lake (kutanthauza kuti wachita ntchito zabwino zomwe ndi Chiyambi cha zabwino Zathu.
Read More »21. Sisitani (kukhula/kutikita ndi dzanja lanu) ziwalo zanu mokwanilira pamene mukusambitsa ndicholinga choti madzi afike paliponse.
22. Ziwalo zonse ziyenera kutsukidwa china pambuyo pachinzake mosachedwetsa.
Read More »Sayyiduna Anas (radhiyallahu anhu) akufotokoza kuti Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) adati, “amene anganditumizire Durood ka 1000 tsiku lachisanu, sadzamwalira kufikira ataonetsedwa malo ake ku Jannah.”
Read More »18. Mukamaliza wudhu, welengeni shahaadah ngati muli malo otakasuka, popanga shahaadah[1] yang’anani kumwamba, momwemonso werengani duwa iliyonse yomwe imabwera m’mahadith. Ena mwamaduwa a sunnah amene anenedwa m’mahadith oyenera kuwerengedwa pamapeto popanga wudhu ndi awa m’musimu: Duwa yoyamba: Amene angawerenge duwa imeneyi makomo asanu ndi atatu a ku Jannah amatseguka kuti …
Read More »Sayyiduna Jaabir (radhiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) adati, "amene angawerenge Durood ka 100 tsiku lirilonse, Allah Ta'ala adzakwaniritsa zofuna zake zokwana 100, 70 adzalandira pa tsiku la Qiyamah ndipo 30 adzapatsidwa padziko pompano.
Read More »