Rasulullah (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam) adampatsa olemekezeka Talhah (radhwiyallahu ‘anhu) dzina loti Al-Fayyaadh (munthu owolowa manja kwambiri) kangapo. Pansipa pali nkhani imodzi yotere: Pankhondo ya Zi Qarad, Rasulullah (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam) adadutsa pachitsime cha Baisaan. Madzi a m’chitsimechi ankadziwika kuti ndi anchere. Rasulullah (Swalla Allaahu …
Read More »Zizindikiro za Qiyaamah 4
Zizindikiro Khumi Zikuluzikulu Za Qiyaamah Monga zilili kuti pali zisonyezo zambiri zing’onozing’ono za Qiyaamah zomwe zalembedwa Mmahaadith, momwemonso pali zisonyezo zikuluzikulu zambiri zomwe zatchulidwanso Mmahaadith. Zizindikiro zikuluzikulu ndi zinthu zofunikira kwambiri zomwe zidzachitike pa dziko lapansi pano Qiyaamah isanafike ndipo zidzalengeza kuyandikira kwa Qiyaamah. Ma Muhadditheen aika kubwera kwa Imam …
Read More »Ma Sunnah Komanso Miyambo Ya Dua 7
18. Popempha mpempheni Mulungu kuti akudalitseni ndi aafiyah (ie kuti akudalitseni momasuka m’magawo onse a moyo wanu). Abbaas (Radhwiyallahu anhu) akusimba kuti: “Nthawi ina ndinamufunsa Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam): “E, Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) wa Allah, ndiphunzitse duwa (yaphindu) imene ndiyenera kupempha kwa Allah. Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) anayankha, “Pemphani …
Read More »Mzake wa Nabi Musah ‘Alaihis Salaam ku Jannah
M’chisilamu ntchito iliyonse yabwino ili ndi kuthekera kolumikizitsa munthu ndi Allah ndikumupezetsa sawabu ku umoyo omwe uli nkudza, komabe pali ntchito zina zimene ndi zapederadera pamanso pa Allah ndipo zimatha kukhala njira yopezera ubwino wa Dini yonse ndi ubwino wa dunya pamodzi. Zina mwa ntchito zimenezo ndi kuonetsa kukoma mtima …
Read More »Olemekezeka Talhah (Radhwiyallahu ‘anhu) Kukwaniritsa Lonjezo Lake
Olemekezeka Talhah (Radhwiyallaahu ‘anhu) akuti: Ma Swahaabah (Radhwiya Allahu ‘anhum) adauza munthu wina okhala kumudzi kuti: “Pita ukafunse kwa Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) kuti Allah Ta’ala akunena za ndani (m’ndime yotsatira ya Quraan Majeed)” (ma Sahaabah) ndi amene adakwaniritsa lonjezo lawo (ndi Allah Ta’ala lokhala okhazikika pankhondo okonzeka kupereka …
Read More »Ma Sunnah Komanso Miyambo Ya Dua 6
16.Lekani kulongosora mwatsatanetsatane pa dua yanu. M’malo mwake, muyenera kupempha zabwino zonse. Nthawi ina Abdullah bin Mughaffal Radhwiyallahu anhu anamva mwana wake akupempha m’mawu otsatirawa: “O Allah! Ndikukupemphani nyumba yachifumu yoyera kumbali yakumanja kwa Jannah ndikalowa m’menemo.” Atamva izi Abdullah bin Mughaffal (Radhwiyallahu anhu) adati: “E, mwana wanga! Mpemphe Allah …
Read More »Olemekezeka Talhah (Radhiyallahu ‘anhu) pa Nkhondo ya Uhud
Olemekezeka Jaabir bin Abdillah (Radhwiya Allaahu ‘anhu) adati: Pa tsiku la nkhkndo ya Uhud, pamene ma Swahaabah adayamba kuthawa kunkhondo, Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) adasiidwa yekha pamalo ena ndi ma Swahaaba khumi ndi awiri okha.) Ma mushrikiin atapita kwa Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) ndi ma Swahaabah khumi ndi …
Read More »Chisilamu cha Olemekezeka Talhah bin Ubaidillah (Radhwiyallahu ‘anhu)
Tsiku lomwe sayyiduna Abu Bakr Siddeeq (Radhwiyallahu ‘anhu) adalowa Chisilamu, adayamba kuyitanira anthu ku Chisilamu, Allah Ta’ala adamupanga kukhala njira ya ma Swahaabah (radhwiyallahu ‘anhun) ambiri kulowa Chisilamu. Mwa ma Swahaabah amene adalowa Chisilamu kudzera mwa Abu Bakr Siddeeq (radhwiyallahu ‘anhu) anali Talhah bin Ubaidillah (radhwiyallahu ‘anhu). Talhah (radhwiyallahu ‘anhu) …
Read More »Kuolowa Manja kwa Olemekezeka Talhah (Radhwiyallahu ‘anhu)
Ali bin Zayd (Rahimahullah) akusimba kuti nthawi ina yake, Nchikumbe wina adapita kwa Talhah (Radhwiyallahu ‘anhu) kuti akapemphe thandizo kwa iye. Nchikumbeyu kudapezeka zoti adali m’bale wake wa Talhah (Radhwiyallahu ‘anhu) ndipo popereka pempho lake, adamupempha kudzera mu ubale omwe udalipo pakati pawo. Talha (Radhwiya Allaahu ‘anhu) adayankha: “Kupatula Inu, …
Read More »Zizindikiro za Qiyaamah 3
Zizindikiro Zing’onozing’ono kuchuluka Pambuyo pa Zizindikiro Zikuluzikulu Ukawona zisonyezo zing’onozing’ono za Qiyaamah zomwe zidalembedwa Mmahaadith, munthu atha kuzindikira kuti ndi chiyambi cha kubwera kwa zisonyezo zikuluzikulu. Choncho, zoona zake ndi zoti, zizindikiro zing’onozing’ono zizidzaonjezereka pang’onopang’ono, mpaka pamapeto pake, zidzafika pachimake pa kubwera kwa zizindikiro zikuluzikulu. M’mahadith ena, Mtumiki (Swalla Allaahu …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu