14. Amene wayambilira kupereka salaam amalandira Malipiro ochuluka. Abu Umaamah radhwiyallahu anhu wanena kuti Mtumiki swallallahu alaihi wasallam adati: “Amene amayambilira kuwalonjera anthu ena popereka salaamu amadziyandikitsa chifupi kwambiri mwa iwo kwa Allah (amakhala pafupi kwambiri ndi chifundo cha Allah). 15. Munthu akakupatsirani salaamu ya munthu, muyankhe ponena kuti “Alaikum …
Read More »Sunnats Ndi Aadaab Za Salaam 5
12. Pangani salaam polowa m’nyumba. Ngati m’nyumba mulibe aliyense, muyenera kupereka salaamu ponena kuti: السَّلَامُ عَلَيْنَا وَعَلَى عِبَادِ اللَّهِ الصَّالِحِينَ Mtendere ukhale pa ife ndi pa akapolo abwino a Allah. Olemekezeka Anas radhwiyallahu anhu adati: nthawi ina Rasulullah swallallahu alaihi wasallam adandiuza kuti: “E iwe mwana wanga okondedwa,ukamalowa m’nyumba mwako, …
Read More »Sunnats Ndi Aadaab Za Salaam 4
9. Mawu a salaam amathera ndi “Wa barakaatuhu”. Munthu asawonjezere mau ena pambuyo pa “Wa barakaatuhu” Muhammad bin Amr bin Ataa rahimahu-Allah adanena kuti: Nthawi ina ndidali chikhalire ndi Abdullah bin Abbaas radhwiyallahu anhu pamene munthu wina ochokera ku Yemen adafika pamalopa ndipo adapereka salaam kuti: “Assalaamu alaikum wa rahmatullahi …
Read More »Sunnats Ndi Aadaab Za Salaam 3
6.Ziri Makruhu kupereka salaam kwa munghu yemwe watangwanika ndi ntchito ina ya Dini kapena akudya. 7. Musapereke salaam kwa omwe sali Mahram (Siwachibale). Ngati mkazi yemwe sali Mahram wapereka salaamu kwa mwamuna, koma kuti okalamba, ndipo palibe kuopa fitnah, akhonza kuyankhidwa. Komabe, ngati ndi mtsikana akupanga salaam, ndiye kuti munthu …
Read More »Sunnats Ndi Aadaab Za Salaam 2
3. Njira ya Sunnat yakaperekedwe ka salaam ndi kupereka moni kwa Asilamu onse, osati achibale ake, abwenzi ake ndi amene akuwadziwa okha. Olemekezeka Abdullah bin Amr radhwiyallahu anhu akusimba kuti munthu wina adamufunsa Mtumiki Swallallahu alaihi wasallam “Kodi ndi chikhalidwe chanji ndi mChisilamu chomwe chili choyamikirika komanso chabwino?” Adayankha Mtumiki …
Read More »Sunnats Ndi Aadaab Za Salaam 1
1. Ukakumana ndi Msilamu nzako, mupatse salaamu. Olemekezeka Ali radhwiyallahu anhu akunena kuti Mtumiki (Swallallahu alaihi wasallam) adati: “Msilamu ali ndi ma ufulu asanu ndi umodzi pa Msilamu nzake. Akakumana naye amlonjere (ndi salamu); ngati amuitana avomere kuitana kwake; akayetsemula amupangire duwa ponena kuti. ‘Yarhamukallah’ akadwala azikamuona akamwalira aziperekeza nawo …
Read More »Ma Ubwino Okhudza Kupereka Salaam
Ubwino Oyambilira kupanga Salaam Olemekezeka Abdullah bun Masuud (Allah asangalale naye) akusimba kuti Rasulullah (madalitso ndi mtendere zikhale pa iye) adati: “Amene amayambilira kupereka Salaam ndi osadzitukumura.”[1] Njira Yokhanzikitsira Chikondi Olemekezeka Abu Hurairah (Allah asangalare naye) akusimba kuti Rasulullah (madalitso ndi mtendere zipite kwa iye) adati: “Simudzalowa ku Paradiso pokhapokha …
Read More »Salaam
Salaam ndi moni wa Chisilamu. Monga momwe Chisilamu chimatanthauza mtendere, moni wa Chisilamu ndi moni wamtendere komanso ofalitsa uthenga wamtendere. Salaam ndi imodzi mwa zochitika zachisilamu zomwe ndi chizindikiro cha Msilamu, ndipo kufunika kwake kwatsindikitsidwa kwambiri mahadith. Olemekezeka Abdullah bin Salaam (Radhwiyallahuanhu) akuti: Mtumiki (madalitso ndi mtendere zikhale pa iye) …
Read More »Kutonthoza Oferedwa
13. Sizoloredwa kupita ku nyumba ya kafiri yemwe wamwalira kukapepesa mwambo wamaliro uli mkati. Koma akakhala kuti ndi kafiri oyandikana naye nyumba kapena kaafir aliyense amene wataya wachibale wake, mwachitsanzo, mwana, ukhoza kumutonthoza ndi mawu awa: أَخْلَفَ اللّه عَلَيْكَ خَيْرًا مِنْهُوَاَصْلَحَكَ Akhlafa Allahu ‘Alayka Khayran Minhu Wa ‘Aslahaka Allah akupatse …
Read More »Kutonthoza Oferedwa
7. Nkoloredwa kuyamikira omwalirayo. Komabe, pomutamanda, onetsetsani kuti simukukokomeza kapena kumutamanda pa makharidwe amene panalibe mwa iye. Momwemonso musatengere chikharidwe ndi njira za makafiri pomutamanda. 8. kuchuluka kwa nthawi ya ta’ziyat ndi masiku atatu kuchokera tsiku lomwalira. Pambuyo pa tsiku lachitatu, ndi makruh kupanga ta’ziyat. Komabe, ngati munthu sadathe kubwera …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu