admin

Ruku Ndi I’tidaal

1. Mukamaliza kuwerenga Surah Faatihah ndi surah ina, yimani kaye pang’ono ndipo kenako kwezani manja anu (monga momwe tafotokozera mu takbeeratul ihraam) uku mukunena takbira ndi kupita pa rukuu.”[1] Zindikirani: Takbeeraat intiqaaliyyah (takbira yomwe imanenedwa posuntha kuchoka ku kaimidwe kena kupita ku kena) iyenera kuyambika munthu akangoyamba kusuntha kupita ku …

Read More »

Munthu Wabwino Kwambiri pa Ummah uwu

Hazrat Abu Dardaa radhiyallah anhu wanena kuti: “Nthaŵi ina yake, Mtumiki (Swallallaahu alaih wasallam). adandiona ndikuyenda kutsogolo kwa Hazrat Abu Bakr (Radhiyallahu ‘anhu) “Pamene Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wa sallam) adaona izi, adandiuza kuti: “Usayende kutsogolo kwa amene ali wabwino kuposa iwe. Pambuyo pake Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi …

Read More »

Kulemba Durood pa kutha kolemba dzina la Mtumiki swallallahu alaih wasallam

عن أبي هريرة قال: قال رسول الله صلى الله عليه وسلم: من صلى علي في كتاب لم تزل الملائكة تستغفر له ما دام اسمي في ذلك الكتاب (المعجم الأوسط للطبراني، الرقم: 1835، وسنده ضعيف كما في كشف الخفاء، الرقم: 2518) Olemekezeka Abu Hurairah (radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (swallallahu alaih …

Read More »

Qiyaam

12. Kenako udzayamba kuwerenga surah Faatihah ndi surah ina kapena gawo lina la Quraan Majeed. Musanayambe kuwerenga surah faatihah, werengani tasmiyah chifukwa ndi gawo la surah fatihah. Tasmiyah ndi kuwerenga: بسم اللهِ الرَّحْمنِ الرَّحِيمِ M’dzina la Allah, Wachifundo chambiri, Wachisoni. Dziwani izi: Ngati ndiwe Imaam, werenga tasmiyah mokweza mu Swalaah …

Read More »

Hazrat Abu Bakr Siddeeq (Radhwiyallahu ‘anhu) ali m’phanga la Thaur

Ali kuphangako paulendo wa Hijrah, zikunenedwa kuti Hazrat Abu Bakr Siddeeq (radhwiyallahu anhu) adali ndi nkhawa kuti palibe cholengedwa chomwe chingatuluke mu dzenje lililonse la mphangamo ndi kuvulaza Hazrat Rasulullah (Swallallaahu ‘alayhi wasallam). Choncho, anayamba kutseka mabowo onse a m’phangamo ndi zidutswa za malaya ake apansi. Komabe, padali mabowo awiri …

Read More »

Tafseer of Surah Kauthar

Ndithu, Ife takupatsa (ndi kukudalitsa) zabwino zambiri Choncho pemphera Swala kwa Mbuye wako, ndipo pereka nsembe. Ndithu, amene akudana nawe adzadulidwa.

M’surayi Allah Ta’ala akulankhula ndi Mtumiki (Swallallaahu ‘alayhi wasallam) kuti: “Ndithu, Ife takupatsa (ndipo takudalitsa ndi) zabwino zambiri.

Zabwino zochuluka zomwe Hazrat Rasulullah (Swallallaahu 'alayhi wasallam) adadalitsidwa nazo padziko lapansi zikuoneka kudzera mu dzina lake la Mubaarak ndi kukwezedwa ulemu, chipembedzo chake chikupitilira kutukuka ndikukula mphamvu ndi mphamvu, ndi kuchuluka kwa anthu olowa m'chipembedzo cha Allah. Chisilamu chikuchuluka tsiku ndi tsiku.

Read More »

Qiyaam

10. Mukangoiyamba swalah yanu werengani Duaa-ul Istiftaa chamuntima. وَجَّهْتُ وَجْهِيَ لِلَّذِيْ فَطَرَ السَّمَاوَاتِ وَالْأَرْضَ حَنِيْفًا مُسْلِمًا وَمَا أَنَا مِنَ الْمُشْرِكِيْنَ إِنَّ صَلَاتِيْ وَنُسُكِيْ وَمَحْيَايَ وَمَمَاتِيْ لِلّٰهِ رَبِّ الْعَالِمِيْنَ لَا شَرِيْكَ لَهُ وَبِذلِكَ أُمِرْتُ وَأَنَا مِنَ الْمُسْلِمِيْنَ Ndikuyang’ana nkhope yanga kwa Yemwe adalenga thambo ndi nthaka, ndikukhala panjira yoongoka popanda kusokonekera, …

Read More »

Olemekezeka Abu Bakr (Radhwiyallahu anhu) Kupereka Chuma Chake Kwa Mtumiki (Swallallaahu ‘alayhi wasallam)

Olemekezeka Abu Hurairah (radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (swallallah alayhi wasallam) adati: “Palibe chuma cha munthu chomwe chidandipindulira monga chuma cha Abu Bakr (radhiyallahu anhu), atamva izi olemekezeka Abu Bakr (radhwiyallahu anhu) adayamba kulira nati: “Chuma changa ndi zonse ndi zanu. Pali nkhani ya olemekezeka Abu Hurairah (radhwiyallahu anhu) m’buku …

Read More »

Kuwerenga Durood Musanapange Dua

عن عبد الله بن مسعود قال إذا أراد أحدكم أن يسأل فليبدأ بالمدحة والثناء على الله بما هو أهله ثم ليصل على النبي صلى الله عليه وسلم ثم ليسأل بعد فإنه أجدر أن ينجح (المعجم الكبير للطبراني، الرقم: 8780، ورجاله رجال الصحيح إلا أن أبا عبيدة لم يسمع من أبيه …

Read More »

Qiyaam

7. Nthawi yowerenga Takbiiratul ihraam (Takbiir-e-Tahriimah) onetsetsani kuti maso anu a kuyang’anaya malo opanga Sajdah ndikupendamitsa mutu wanu pang’ono pansi.[1]  8. Ikani dzanja lanu lamanja pa dzanja lanu lamanzere ndikuwaika pansi pa chidali pamwamba pa nchombo.[2]  9. Gwirani joini yanu ya dzanja lamanzere ndi dzanja lanu lamanja, zala zanu zakumanja …

Read More »