Masunna Ndi Aadaab (Miyambo)

Sajdah

1. Nenani takbira ndikupita pa sajdah. 2. Gwirani manja anu m’mawondo pamene mukupita pa sajdah 3. Choyamba ikani mawondo pansi, kenako zikhatho, ndipo pomalizira pake chipumi ndi mphuno pamodzi. 4. Siyani zala zotsekeka moyang’anitsa ku chibla. 5. Ikani zikhatho zanu pansi m’njira yoti zala zifanane ndi makutu ndipo mbali zigwirizane …

Read More »

Ruku ndi I’tidaal

6. Timisomali tamapazi onse awiri akhale pamodzi. Ngati izi ndizovuta, ndiye kuti ziyenera kusungidwa moyandikana momwe zingathekere(momwe mungakwanitsire). 7. Yang’anani malo a sajdah m’maimidwe a ruku (pamene muli pa ruku). 8. Werengani tasbeeh katatu kapena nambala ina iliyonse yosagawika pawiri.   سُبْحَانَ رَبِّيَ الْعَظِيْم Subhaana rabbiyal A’dhwiim Kuyeretsedwa konse ndi …

Read More »

Ruku ndi I’tidaal

1. Mukamaliza kuwerenga Surah Faatihah ndi surah ina, yimani kaye pang’ono ndipo pambuyo pake kwezani manja (monga momwe tafotokozera mu takbeeratul ihraam) uku mukunena takbira ndikupita pa rukuu. Zindikirani: Takbeeraat intiqaaliyyah (takbeer yomwe imanenedwa posuntha kuchoka ku kaimidwe kena kupita ku kena) iyenera kuyambika munthu akangoyamba kusuntha kupita ku kaimidwe …

Read More »

Qiyaam

10. Mukangoyamba Swalaah, werengani Dua-ul Istiftaah chamuntima: وَجَّهْتُ وَجْهِيَ لِلَّذِيْ فَطَرَ السَّمَاوَاتِ وَالْأَرْضَ حَنِيْفًا مُسْلِمًا وَمَا أَنَا مِنَ الْمُشْرِكِيْنَ إِنَّ صَلَاتِيْ وَنُسُكِيْ وَمَحْيَايَ وَمَمَاتِيْ لله ِرَبِّ الْعَالِمِيْنَ لَا شَرِيْكَ لَهُ وَبِذلِكَ أُمِرْتُ وَأَنَا مِنَ الْمُسْلِمِيْنَ Ndatembenukira nkhope yanga kwa Yemwe adalenga thambo ndi nthaka, ndikukhalabe panjira yoongoka popanda kusokonekera, ndikugonjera …

Read More »

Qiyaam

1. Yang’anani kuchibula. 2. Sungani mapazi pamodzi kapena pafupi momwe mungakwanitsire. Onetsetsani kuti mapazi ayang’ana kuchibla. 3. Pambuyo pake, pangani Niya ya Swalah yomwe mukuswali ndipo kwezani manja anu mpaka zala zanu zazikulu zigwirizane ndi nsonga zamakutu ndipo nsonga za zala zanu zikhale molingana ndi kumtunda kwa makutu anu. 4. …

Read More »

Swalaah Isanayambe

1. Chisamaliro chapadera chiyenera kutengedwa povala moyenera pa Swalaah. Mkazi ayenera kuvala chovala choterocho chomwe chidzabisa thupi lake lonse ndi tsitsi lake. Ndikusadzipatsa ulemu iye mwini kuvala zovala zothina zomwe zimasonyeza mmene thupi lake lilili kapena kuvala zovala zopyapyala zimene zingachititse kuti ziwalo zenizeni ziwonekere. Ngati chovalacho chili chooneka kuti …

Read More »

Mfundo Ya Imaam Shaafi’ee

Imaam Shaafi’e (rahimahullah) walemba mu chitabu chotchedwa Ikhtilaaful Hadith kuti: Sitikudziwa mwa akazi olemekezeka a Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) kusiya nyumba zawo ndikupita kunzikiti kukaswali Swalaah ya Jumuah kapena Swalah ina iliyonse, ngakhale kuti adali akazi olemekezeka a Sayyiduna Rasulullah chifukwa cha udindo wawo wapadera ndi ubale wawo ndi Mtumiki …

Read More »

Kapempheredwe ka Azimayi

Mazhab anayi Kuyambira nthawi ya Sayyiduna Rasulullah, ma Swahaabah, Taabi’een ndi zaka mazana zotsatira, akazi ankalamulidwa kuswali m’njira yosiyana ndi Swalaah ya amuna m’magawo ena za swalah. Madhabu onse anayi (omwe ndi Hanafi, Maliki, Shafi’i ndi Hambali) onse amagwirizana pa mfundo yakuti Swalaah ya akazi imasiyana ndi Swalaah ya amuna …

Read More »

Kapempheredwe ka Azimayi

Chilichonse cha chipembedzo cha Chisilamu chokhudzana ndi akazi chimakhanzikika pa kukhala odzichepetsa komanso wamanyazi. Pachifukwa ichi ndi pamene Chisilamu chikulamula amayi kuti azikhala m’nyumba zawo, kukhala obisika kwa amuna achilendo, komanso kuti asachoke m’nyumba zawo popanda chifukwa chenicheni pa Sharia. M’mene mkazi walamulidwira kuswali Swalah yake – kuyambira pa chovala …

Read More »

Sunna Za Msikiti

37. Ulumikizitseni mtima wanu nthawi zonse ndiku mzikiti. Mwachitsanzo pamene mukuchoka mumzikiti pomwe mwatsiriza swalah yanu, pangani niya kuti mubweranso kumzikitiko paswala yotsatirayo ndipo idikireni swalayo ndimtima onse.[1] عن أبي هريرة رضي الله عنه أن رسول الله صلى الله عليه وسلم قال ألا أدلكم على ما يمحو الله به الخطايا …

Read More »