Kuwerenga Durood Musadayambe Kupanga Duwa

عن عبد الله بن مسعود قال إذا أراد أحدكم أن يسأل فليبدأ بالمدحة والثناء على الله بما هو أهله ثم ليصل على النبي صلى الله عليه وسلم ثم ليسأل بعد فإنه أجدر أن ينجح (المعجم الكبير للطبراني، الرقم: ٨٧٨٠، ورجاله رجال الصحيح إلا أن أبا عبيدة لم يسمع من أبيه …

Read More »

Zikhulupiliro Zokhudza Mtumiki Wa Allah Muhammad (Sallallah alayhi wasallam)

5. Allah Ta’ala adamudalitsa Mtumiki (sallallah alayhi wasallam) ndi zabwino zapadera zimene Atumiki ndi aneneri a Mulungu sadapatsidwe. Mtumiki (salallah alayhi wasallama) akusimba kuti:

(Ndadalitsidwa ndi zinthu zisanu ndi chimodzi (6), zimene atumiki akale sadapatsidwepo, Ndadalitsidwa popatsidwa jawaamil al kalaam (Mau amodzi koma amatanthauzo ochuluka, mwachitsanzo Quran yolemekezeka komanso mahadith olemekezeka muli matanthauzo akuluakulu kuchokera mu mau ochepa),

 

Read More »

Njira Ya Sunnah Yogwiritsira Ntchito Miswaak (mswachi ochokera ku mtengo)

4. Mukatsiriza kugwiritsa ntchito miswaak, utsukeni ndipo uyikeni choimika.[1] 5. Ngati palibe Miswaak, Chala sichingalowe m’malo mwa miswak, Kotero munthu adzayenera kugwiritsa ntchito chinthu chokhuthala chimene chingathe kuyeretsa mkamwa, monga nswachi (toothbrush).[2] 6. Miswaak siwoyenera kuti utali wake upambane chikhatho chadzanja limodzi.[3] 7. Kamtengo kali konse komwe kamakhala bwino kuchukuchira …

Read More »

Zikhulupiliro Zokhudza Mtumiki Wa Allah Muhammad (Sallallah alayhi wasallam)

1. Mtumiki Muhammad (salallah alayhi wasallam) ndi Mtumiki otsirizira mwa atumiki onse a Allah. Palibenso Mtumiki wina yemwe adzatumizidwe padziko lapansi kudzaongolera anthu ku dziko lirilonse. Ngati wina wake ali ndi chikhulupiliro kuti kudzabwera mtumiki wina pambuyo pa Mtumiki Muhammad (salallah alayhi wasallam) munthu ameneyo ndi Kafiri (simsilamu) ndipo wasemphana …

Read More »

Njira Ya Sunnah Yogwiritsira Ntchito Miswaak (mswachi ochokera ku mtengo)

1. Njira yogwilira miswaak ili motere, Munthu ayenere ayike chala chachikulu ndi chaching´ono pansi pa miswaak ndipo zala zake zotsalazo ayike mbali yapamwamba pa Miswaak.[1] 2. Gwirani Miswaak ndi mkono wamanja ndipo yambani kutsuka mano kuyambira mbali yakumanja.[2] 3. Tsukani mano mopingasa ndipo lilime mulitsuke molitsatira (mulitali make), chimodzimodzinso, tsukani …

Read More »