عن عبد الله بن مسعود قال إذا أراد أحدكم أن يسأل فليبدأ بالمدحة والثناء على الله بما هو أهله ثم ليصل على النبي صلى الله عليه وسلم ثم ليسأل بعد فإنه أجدر أن ينجح (المعجم الكبير للطبراني، الرقم: ٨٧٨٠، ورجاله رجال الصحيح إلا أن أبا عبيدة لم يسمع من أبيه …
Read More »Nthawi Zimene Miswak Ikufunika Kugwirtsidwa Ntchito
1. Mukangodzuka kumene.
Sayyiduna Aishah radhiyallahu anha akusimba kuti, nthawi zonse Mtumikisallallahu alaih wasallam ankati akadzuka, kaya ndimasana kapena usiku ankatsuka mkamwa ndi miswak asanapange wudhu.’’
Read More »Zikhulupiliro Zokhudza Mtumiki Wa Allah Muhammad (Sallallah alayhi wasallam)
5. Allah Ta’ala adamudalitsa Mtumiki (sallallah alayhi wasallam) ndi zabwino zapadera zimene Atumiki ndi aneneri a Mulungu sadapatsidwe. Mtumiki (salallah alayhi wasallama) akusimba kuti:
(Ndadalitsidwa ndi zinthu zisanu ndi chimodzi (6), zimene atumiki akale sadapatsidwepo, Ndadalitsidwa popatsidwa jawaamil al kalaam (Mau amodzi koma amatanthauzo ochuluka, mwachitsanzo Quran yolemekezeka komanso mahadith olemekezeka muli matanthauzo akuluakulu kuchokera mu mau ochepa),
Read More »
Kupeza duwa ya Mtumiki (sallallahua alaih wasallam) chifukwa chowerenga Durood pa tsiku la Jumuah
Sayyiduna Umar bin Khattwaab (radhiyallahu anhu) akufotokoza kuti Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) adati: Chulukitsani kundiwerengera Durood pa tsiku la Jumuah popeza Durood yanu imafikitsidwa kwa ine ndipo kenako ndimakupangirani kupempha Allah kuti akukhululukireni machimo anu.
Read More »Njira Ya Sunnah Yogwiritsira Ntchito Miswaak (mswachi ochokera ku mtengo)
4. Mukatsiriza kugwiritsa ntchito miswaak, utsukeni ndipo uyikeni choimika.[1] 5. Ngati palibe Miswaak, Chala sichingalowe m’malo mwa miswak, Kotero munthu adzayenera kugwiritsa ntchito chinthu chokhuthala chimene chingathe kuyeretsa mkamwa, monga nswachi (toothbrush).[2] 6. Miswaak siwoyenera kuti utali wake upambane chikhatho chadzanja limodzi.[3] 7. Kamtengo kali konse komwe kamakhala bwino kuchukuchira …
Read More »Zikhulupiliro Zokhudza Mtumiki Wa Allah Muhammad (Sallallah alayhi wasallam)
1. Mtumiki Muhammad (salallah alayhi wasallam) ndi Mtumiki otsirizira mwa atumiki onse a Allah. Palibenso Mtumiki wina yemwe adzatumizidwe padziko lapansi kudzaongolera anthu ku dziko lirilonse. Ngati wina wake ali ndi chikhulupiliro kuti kudzabwera mtumiki wina pambuyo pa Mtumiki Muhammad (salallah alayhi wasallam) munthu ameneyo ndi Kafiri (simsilamu) ndipo wasemphana …
Read More »Maduwa aimitsidwa kufikira durood itawerengedwa
Sayyiduna Umar (radhiyallahu anhu) akusimba kuti, maduwa amatsakamira m’lengalenga. Samadutsa kupita kumwamba ngati durood siikutumizidwa kwa Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) (palibe galantidi yoti duwayo ilandiridwa).
Read More »Njira Ya Sunnah Yogwiritsira Ntchito Miswaak (mswachi ochokera ku mtengo)
1. Njira yogwilira miswaak ili motere, Munthu ayenere ayike chala chachikulu ndi chaching´ono pansi pa miswaak ndipo zala zake zotsalazo ayike mbali yapamwamba pa Miswaak.[1] 2. Gwirani Miswaak ndi mkono wamanja ndipo yambani kutsuka mano kuyambira mbali yakumanja.[2] 3. Tsukani mano mopingasa ndipo lilime mulitsuke molitsatira (mulitali make), chimodzimodzinso, tsukani …
Read More »Mmene Allah Taala Amazisamalilira Zolengedwa Zake
6. Chigamulo cha Allah chilichonse muli nzeru ndiluntha ngakhalebe munthu samatha kumvetsa zolinga za Allah Ta'ala. Choncho munthu akuyenera kumvetsa ndi kusangalala ndi Chigamulo cha Allah Ta’ala nthawi zonse.
Read More »Mtumiki (Sallallahu Alaih Wasallam) Kumpemphera Munthu Chikhululuko
Sayyiduna Umar bin Khattwaab (radhiyallahu anhu) akufotokoza kuti Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) adati, Chulukitsani kundiwerengera Durood usiku ndi Usana wa tsiku la Jumuah (lachisanu) chifukwa Durood yanuyo imandipeza ndipo ndimakupangirani duwa kukupempherani chikhululuko kwa Allah ku machimo anu.
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu