Salaah Ya Amuna

Udindo wapamwamba womwe Swalah ili nawo m’moyo wa Msilamu siufunikira kufotokoza kulikonse. Mfundo yoti idzakhala gawo loyamba lomwe adzafunsidwe munthu pa tsiku la Qiyaamah ndi umboni wokwanira wotsimikizira kufunika kwake. Sayyiduna Rasulullah (swallallahu alaih wasallam) إن أول ما يحاسب الناس به يوم القيامة من أعمالهم الصلاة قال يقول ربنا جل …

Read More »

Chikondi Cha Sahabah wina pa Mtumiki (sallallahu alaih wasallam)

Sahabah wina adabwera kwa Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) ndikufuna kuti oh Mthenga wa Allah kodi Qiyamah idzafika liti? Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) adayankha pomufunsa kuti ndichani chomwe wachita sochinyeza kuikonzekera tsikulo? Sahabah adayankha nati, Oh Mthenga wa Allah sindikudzitenga kuti ndiri ndi swalah Saum kapena sadaqah zochuluka zomwe ndapanga komanso …

Read More »

Tafseer Ya Surah Feel

Kodi siudaone momwe Mbuye wako adawachitira anthu a Njovu? Kodi sadawaononge chiwembu chawo? Ndipo adawatumizira magulu ambalame mmagulumagulu otsatizana, ndikumawagenda ndi miyala yamoto; ndipo adawachita kukhala ngati mmera otafunidwatafunidwa ndiye walavuridwa.

Read More »

Machimo a Zaka Makumi asanu ndi atatu Akhululukidwa, sawabu za Zaka Makumi asanu ndi atatu Zilembedwa Kupyolera mu Kubwereza Durood Makumi asanu ndi atatu tsiku Lachisanu

Hazrat Abu Hurairah (radhwiyallahu anhu) akufotokoza kuti Hazrat Rasulullah (swallallahu alaih wasallam) adati "kundiwerengera Duruud kudzakhala kuwala pa Mlatho (Paul-Siraat) ndipo amene adzandiwerengere Duruud tsiku lachisanu kokwana makumi asanu ndi atatu (80), adzakhululukidwa zaka makumi asanu ndi atatu za machimo ake."

Read More »

Sunna Za Msikiti

37. Ulumikizitseni mtima wanu nthawi zonse ndiku mzikiti. Mwachitsanzo pamene mukuchoka mumzikiti pomwe mwatsiriza swalah yanu, pangani niya kuti mubweranso kumzikitiko paswala yotsatirayo ndipo idikireni swalayo ndimtima onse.[1] عن أبي هريرة رضي الله عنه أن رسول الله صلى الله عليه وسلم قال ألا أدلكم على ما يمحو الله به الخطايا …

Read More »

Chikondi chomwe Zaid bin Dhathinah (radhiyallahu anhu) ankamuonetsera Mtumiki (sallallahu alaih wasallam)

Makafiri ali pafupi kuti amuphe sahabah Olemekezeka Zaid bin Dhathinah (radhiyallahu anhu) adamufunsa kuti ungasangalale kuti m’malo mwako timuphe Muhammad ndikuti iweyo tikusiye udzikasangalala ndi banja lako? Yankho lake lodabwitsa lidali loti ndikulumbira mwa Allah sindingalore kuti ine ndikhale ndi banja langa kumasangalala ndipo Muhammad akuvutika ngakhale kutakhala kubaidwa ndi …

Read More »

Machimo a Zaka Makumi asanu ndi atatu Akhululukidwa, sawabu za Zaka Makumi asanu ndi atatu Zilembedwa Kupyolera mu Kubwereza Durood Makumi asanu ndi atatu tsiku Lachisanu.

وعن سهل بن عبد الله قال من قال في يوم الجمعة بعد العصر اللهم صل على محمد النبي الأمي وعلى إله وسلم ثمانين مرة غفرت له ذنوب ثمانين عاماً أخرجه ابن بشكوال وقد تقدم قريباً في حديث أبي هريرة معناه (القول البديع صـ 400) Zidanenedwa ndi Hazrat Sahl bun Abdullah …

Read More »

Sunna Za Msikiti

34. Kutha kwa Adhana, ngati sudapemphere swalah, usatuluke mumzikiti pokhapokha patakhala zifukwa zomveka bwino.[1] عن أبي الشعثاء قال كنا قعودا في المسجد مع أبي هريرة رضي الله عنه فأذن المؤذن فقام رجل من المسجد يمشي فأتبعه أبو هريرة رضي الله عنه بصره حتى خرج من المسجد فقال أبو هريرة رضي …

Read More »

Sayyiduna Abu Ubaidah (radhiyallahu) anhu aluza mano ake

Pankhondo ya Uhud Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) adavulazidwa kwambiri ndi adani ndipo zitsulo za chipewa chake chodzitetezera pa nkhondo zinabaya pankhope yake yolemekezeka. Sayyiduna Abu Bakr Siddiq komanso Abu Ubaidah (Radhiyallahu anhuma) adathamangira kukamuthandizira Rasulullah (sallallahu alaih wasallam). Sayyiduna abu Ubaidah (radhiyallahu anhu) atafika pamene panali Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) …

Read More »

Tafseer Ya Surah Humazah

Tsoka kwa aliyense ochita miseche, wonyoza, wodziunjikira chuma ndikuchiwerengera! Akuganiza kuti chuma chake chidzamkhazika muyaya. Ayi! Ndithu, adzaponyedwa ku Hutwamah (kumoto waukali). Ndipo nchiyani chingakudziwitse kuti 'Hutamah' ndi chiyani? Ndi moto wa Allah woyatsidwa umene uzidzalowa m’mitima mwawo. (Motowo) udzatchingidwa ndi zipupa zitalizitali, ndi mizati yotambasulidwa (yotambasuka).

Read More »