Kodi siudaone momwe Mbuye wako adawachitira anthu a Njovu? Kodi sadawaononge chiwembu chawo? Ndipo adawatumizira magulu ambalame mmagulumagulu otsatizana, ndikumawagenda ndi miyala yamoto; ndipo adawachita kukhala ngati mmera otafunidwatafunidwa ndiye walavuridwa.
Read More »Machimo a Zaka Makumi asanu ndi atatu Akhululukidwa, sawabu za Zaka Makumi asanu ndi atatu Zilembedwa Kupyolera mu Kubwereza Durood Makumi asanu ndi atatu tsiku Lachisanu
Hazrat Abu Hurairah (radhwiyallahu anhu) akufotokoza kuti Hazrat Rasulullah (swallallahu alaih wasallam) adati "kundiwerengera Duruud kudzakhala kuwala pa Mlatho (Paul-Siraat) ndipo amene adzandiwerengere Duruud tsiku lachisanu kokwana makumi asanu ndi atatu (80), adzakhululukidwa zaka makumi asanu ndi atatu za machimo ake."
Read More »Sunna Za Msikiti
37. Ulumikizitseni mtima wanu nthawi zonse ndiku mzikiti. Mwachitsanzo pamene mukuchoka mumzikiti pomwe mwatsiriza swalah yanu, pangani niya kuti mubweranso kumzikitiko paswala yotsatirayo ndipo idikireni swalayo ndimtima onse.[1] عن أبي هريرة رضي الله عنه أن رسول الله صلى الله عليه وسلم قال ألا أدلكم على ما يمحو الله به الخطايا …
Read More »Chikondi chomwe Zaid bin Dhathinah (radhiyallahu anhu) ankamuonetsera Mtumiki (sallallahu alaih wasallam)
Makafiri ali pafupi kuti amuphe sahabah Olemekezeka Zaid bin Dhathinah (radhiyallahu anhu) adamufunsa kuti ungasangalale kuti m’malo mwako timuphe Muhammad ndikuti iweyo tikusiye udzikasangalala ndi banja lako? Yankho lake lodabwitsa lidali loti ndikulumbira mwa Allah sindingalore kuti ine ndikhale ndi banja langa kumasangalala ndipo Muhammad akuvutika ngakhale kutakhala kubaidwa ndi …
Read More »Machimo a Zaka Makumi asanu ndi atatu Akhululukidwa, sawabu za Zaka Makumi asanu ndi atatu Zilembedwa Kupyolera mu Kubwereza Durood Makumi asanu ndi atatu tsiku Lachisanu.
وعن سهل بن عبد الله قال من قال في يوم الجمعة بعد العصر اللهم صل على محمد النبي الأمي وعلى إله وسلم ثمانين مرة غفرت له ذنوب ثمانين عاماً أخرجه ابن بشكوال وقد تقدم قريباً في حديث أبي هريرة معناه (القول البديع صـ 400) Zidanenedwa ndi Hazrat Sahl bun Abdullah …
Read More »Sunna Za Msikiti
34. Kutha kwa Adhana, ngati sudapemphere swalah, usatuluke mumzikiti pokhapokha patakhala zifukwa zomveka bwino.[1] عن أبي الشعثاء قال كنا قعودا في المسجد مع أبي هريرة رضي الله عنه فأذن المؤذن فقام رجل من المسجد يمشي فأتبعه أبو هريرة رضي الله عنه بصره حتى خرج من المسجد فقال أبو هريرة رضي …
Read More »Sayyiduna Abu Ubaidah (radhiyallahu) anhu aluza mano ake
Pankhondo ya Uhud Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) adavulazidwa kwambiri ndi adani ndipo zitsulo za chipewa chake chodzitetezera pa nkhondo zinabaya pankhope yake yolemekezeka. Sayyiduna Abu Bakr Siddiq komanso Abu Ubaidah (Radhiyallahu anhuma) adathamangira kukamuthandizira Rasulullah (sallallahu alaih wasallam). Sayyiduna abu Ubaidah (radhiyallahu anhu) atafika pamene panali Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) …
Read More »Tafseer Ya Surah Humazah
Tsoka kwa aliyense ochita miseche, wonyoza, wodziunjikira chuma ndikuchiwerengera! Akuganiza kuti chuma chake chidzamkhazika muyaya. Ayi! Ndithu, adzaponyedwa ku Hutwamah (kumoto waukali). Ndipo nchiyani chingakudziwitse kuti 'Hutamah' ndi chiyani? Ndi moto wa Allah woyatsidwa umene uzidzalowa m’mitima mwawo. (Motowo) udzatchingidwa ndi zipupa zitalizitali, ndi mizati yotambasulidwa (yotambasuka).
Read More »Masunnah Ochita Mumzikiti
31. Kupatula kupita kumzikiti kukapemphera, ngati kuli mtsonkhano omwe ukupangidwira mumzikiti, mukuyenera kupanga niya kuti mukupita kumzikiti kukaphunzira za Dini. Ngati wina angakwanitse kuphunzitsa dini choncho akuyenera kupanga niya kuti akubwera kumzikiti kukaphunzitsa dini. عن أبي هريرة رضي الله عنه قال سمعت رسول الله صلى الله عليه وسلم يقول من …
Read More »Kukhudzidwa Kwa Mzimayi Wachi Answaari Pa Nkhani Ya Nabi (Sallallahu Alaih Wasallam)
Ku nkhondo ya Uhud asilamu adavutika kwambiri ndi kugonja komanso asilamu ambiri adaphedwa. Pamene nkhani yokhudzana ndi asilikali akunkhondo aja inawapeza anthu a ku Madina, amayi adatuluka m’nyumba zawo kufuna kudziwa m’mene nkhondo imayendera. Pamene anthu ena adakasonkhana pa malo ena ake mzimayi m’modzi wachi Ansaar adafunsa modandaula kuti kodi …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu