Ruku ndi I’tidaal

6. Timisomali tamapazi onse awiri akhale pamodzi. Ngati izi ndizovuta, ndiye kuti ziyenera kusungidwa moyandikana momwe zingathekere(momwe mungakwanitsire). 7. Yang’anani malo a sajdah m’maimidwe a ruku (pamene muli pa ruku). 8. Werengani tasbeeh katatu kapena nambala ina iliyonse yosagawika pawiri.   سُبْحَانَ رَبِّيَ الْعَظِيْم Subhaana rabbiyal A’dhwiim Kuyeretsedwa konse ndi …

Read More »

Nkhani Zabwino Za Jannah

Sayyiduna Abu Muusa (Radhwiya Allaahu ‘anhu) akufotokoza motere: Tsiku lina ndidali limodzi ndiMtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) mu umodzi mwa minda ya zipatso zaku Madinah Munawwarah pamene munthu wina adadza napempha chilorezo cholowa m’mundawu, atamva pempho la munthuyo, Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wasallam) anandiuza. “Mlole alowe ndikumuwuza nkhani yabwino yokhala …

Read More »

Ruku ndi I’tidaal

1. Mukamaliza kuwerenga Surah Faatihah ndi surah ina, yimani kaye pang’ono ndipo pambuyo pake kwezani manja (monga momwe tafotokozera mu takbeeratul ihraam) uku mukunena takbira ndikupita pa rukuu. Zindikirani: Takbeeraat intiqaaliyyah (takbeer yomwe imanenedwa posuntha kuchoka ku kaimidwe kena kupita ku kena) iyenera kuyambika munthu akangoyamba kusuntha kupita ku kaimidwe …

Read More »

Msilamu Woyamba Kuchita Hijrah (kusamuka) ndi Banja Lake

Olemekezeka Anas (radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Uthmaan (radhwiyallahu anhu) adanyamuka kupita ku Abyssinia, kusamuka ndi mkazi wake olemekezeka, Bibi Ruqayyah (radhwiyallahu anha), mwana wamkazi wodalitsika wa Rasulullah (swallallaahu alaih wasallam). Nkhani zokhudza momwe amakhalira zidachedwa, choncho Mtumiki (sallallahu alaih wasallam) adali ndi nkhawa ndipo amatuluka ku Makka Mukarramah kufuna kudziwa …

Read More »

Qiyaam

10. Mukangoyamba Swalaah, werengani Dua-ul Istiftaah chamuntima: وَجَّهْتُ وَجْهِيَ لِلَّذِيْ فَطَرَ السَّمَاوَاتِ وَالْأَرْضَ حَنِيْفًا مُسْلِمًا وَمَا أَنَا مِنَ الْمُشْرِكِيْنَ إِنَّ صَلَاتِيْ وَنُسُكِيْ وَمَحْيَايَ وَمَمَاتِيْ لله ِرَبِّ الْعَالِمِيْنَ لَا شَرِيْكَ لَهُ وَبِذلِكَ أُمِرْتُ وَأَنَا مِنَ الْمُسْلِمِيْنَ Ndatembenukira nkhope yanga kwa Yemwe adalenga thambo ndi nthaka, ndikukhalabe panjira yoongoka popanda kusokonekera, ndikugonjera …

Read More »

Kugula Chitsime ku Jannah

Pamene Masahaabah (radhiyallahu ‘anhum) adasamukira ku Madinah Munawwarah, madzi omwe adawapeza kumeneko adali ovuta kwa iwo kumwa popeza adali anchere. Komabe, padali Myuda wina yemwe amakhala ku Madinah Munawaarah yemwe adali ndi chitsime chamadzi okoma otchedwa Ruumah, ndipo ankagulitsa madzi a pachitsime chakewo kwa maswahaabah (radhiyallahu ‘anhum). Mtumiki (swallallaahu ‘alayhi …

Read More »

Qiyaam

1. Yang’anani kuchibula. 2. Sungani mapazi pamodzi kapena pafupi momwe mungakwanitsire. Onetsetsani kuti mapazi ayang’ana kuchibla. 3. Pambuyo pake, pangani Niya ya Swalah yomwe mukuswali ndipo kwezani manja anu mpaka zala zanu zazikulu zigwirizane ndi nsonga zamakutu ndipo nsonga za zala zanu zikhale molingana ndi kumtunda kwa makutu anu. 4. …

Read More »

Sayyiduna Umar (Radhiyallahu ‘anhu) Kulamula Zabwino Panthawi Yotsiriza (yamoyo wake)

M’mawa wa tsiku limene Sayyiduna Umar (Radhwiya Allahu ‘anhu) adabayidwa, mnyamata wina adamuyendera nati kwa iye: “Ameer-ul-Mu’mineen! Sangalalani ndi nkhani yabwino yochokera kwa Allah Ta’alal, Inu ndinu Sahaabi wa Mtumiki (Swallallaahu ‘alayhi wasallam) Ndipo inu muli m’gulu la anthu amene adalandira Chisilamu m’masiku oyambirira, ndipo mudasankhidwa kukhala Khalifa ndipo mudachita …

Read More »

Tafseer ya Surah Ikhlaas

بِسْمِ اللَّهِ الرَّحْمَٰنِ الرَّحِيمِ قُلْ هُوَ اللَّهُ أَحَدٌ ‎﴿١﴾‏ اللَّهُ الصَّمَدُ ‎﴿٢﴾‏ لَمْ يَلِدْ وَلَمْ يُولَدْ ‎﴿٣﴾‏ وَلَمْ يَكُن لَّهُ كُفُوًا أَحَدٌ ‎﴿٤﴾‏ Sura iyi ikufotokoza za chikhulupiriro cha Tawhiyd (umodzi wa Allah Ta’ala mu kakharidwe kake ndi mbiri zake), zomwe ndi gawo limodzi lofunikira kwambiri m’zikhulupiliro zazikulu za Chisilamu. Chikhulupiriro cha Tawheed chinali chinthu chachilendo kwa …

Read More »

Swalaah Isanayambe

1. Chisamaliro chapadera chiyenera kutengedwa povala moyenera pa Swalaah. Mkazi ayenera kuvala chovala choterocho chomwe chidzabisa thupi lake lonse ndi tsitsi lake. Ndikusadzipatsa ulemu iye mwini kuvala zovala zothina zomwe zimasonyeza mmene thupi lake lilili kapena kuvala zovala zopyapyala zimene zingachititse kuti ziwalo zenizeni ziwonekere. Ngati chovalacho chili chooneka kuti …

Read More »