Dongosolo la Allah Ta‘ala, kukamba momwe amalengedwera anthu, ndilakuti anthu awiri akakumana munthu amapangidwa. Chinthu choyamba ndi kudzera mwa makolo omwe mbewu ya mwamuna imabzalidwa m’mimba mwa mayi. Chinthu chachiwiri ndi mzimu omwe umalowa m’mimba mwa mwana yemwe sanabadweyo akakwanitsa miyezi inayi. Munthu aliyense amene anabwera padziko lapansi adatsatira njira …
Read More »Yearly Archives: 2026
Akazi Kuphunzira Maphunziro 2
Abdullah bin Mas’uud (radhwiyallahu ‘anhu)
Olemekezeka Abdullah bin Mas’uud (radhwiyallahu ‘anhu) anali mnyamata wamng’ono, akuweta mbuzi za Uqbah bin Abi Mu’ait m’chigawo cha Makkah Mukarramah. Tsiku lina ali kuweta mbuzi, Rasulullah (sallallahu ‘alaihi wasallam) ndi Abu Bakr (radhwiyallahu ‘anhu) adadutsa pamene ankathawa ma mushrikiin. Popeza chinali chizolowezi cha Aarabu kupereka mkaka kwa odutsa mnjira, Rasulullah …
Read More »Masunnah Ndi Miyambo Ya Pakudya 2
Ma Sunnah ndi Miyambo Musanadye 5. Sambani m’manja musanayambe kudya. Olemekezeka Abdullah bin Abbaas (radhwiyallahu anhuma) akusimba kuti Rasulullah (swallallahu alaihi wasallam) adati: Kusamba m’manja usanayambe kudya komanso ukamaliza kumachotsa umphawi, ndipo ndi zochokera mu sunnah ya Ambiya onse (alaihimus salaam). 6. Ndibwino kuti kuvula nsapato usanayambe kudya. Olemekezeka Anas …
Read More »Kufunira Ena Zabwino
Kuchokera mu dongosolo lonse la makhalidwe abwino la Chisilamu, makhalidwe onse omwe Chisilamu chimalimbikitsa ndi odzadza ndi zokopa ndipo amawalitsa kukongola. Kaya ndi kulemekeza okalamba, kapena kuchitira chifundo achinyamata, kapena kukwaniritsa ufulu wa makolo ndi abale anu, zonse zimasonyeza ulemerero wapadera wa Chisilamu. Komabe, moyo wa makhalidwe onse apamwambawa uli …
Read More »Akazi Kuphunzira Maphunziro
Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wa sallam) Kuyamikira Kuwerenga Quran kwa Abdullah bin Mas’uud (Radhwiyallahu ‘anhu)
Umar (radhwiyallahu ‘anhu) adafotokoza nkhani iyi: Rasulullah (swallallahu ‘alayhi wasallam) ankakonda kulankhula ndi Abu Bakr (radhwiyallahu ‘anhu) akamaliza kuswali Esha ndikukambirana naye zokhuza Asilamu. Usiku wina, atamilza swalah ya Esha, Rasulullah (sallallahu ‘alayhi wasallam) adayamba kuyankhula ndi Abu Bakr (radhwiyallahu ‘anhu) (zokhudza Asilamu) ndipo inenso ndidali nawo pomwepo. Pambuyo pokambirana, …
Read More »Nabi Isah ‘alaihis salaaam
Isa (‘alaihis salaam) ndi Mtumiki wa Allah Ta‘ala ndipo ali m’gulu la Aneneri apamwamba. Allah Ta‘ala adamuvumbulutsira Injeel (Baibulo) ndipo adamudaritsa ndi Shari’ah. Iye ndi Nabi amene anatumizidwa padziko lapansi Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) asanabwere. Rasulullah (swallallahu ‘alaihi wasallam) adati, “Ambiyaa onse (‘alaihimus salaam) ali ngati ana a bambo m’modzi. …
Read More »Kudya
Chisilamu ndi Dini ya padziko lonse. Ndi ya nthawi zonse, malo onse ndi anthu onse. Ndi yangwiro komanso yokwanira, kotero kuti yamuonetsa munthu njira yokwaniritsira malamulo a Allah ndi ufulu wa akapolo ake. Munthu asadafike m’dziko kufikira kumwalira, Chisilamu chakhazikitsa malamulo ndi ziletso zomwe zingamuchititse kuti akhale osangalala. Kupatura kupemphera …
Read More »Abu Zar (radhiyallahu ‘anhu) Apereka Uphungu kwa Mtsogoleri wa Asilikali Kuti Atsatire Chilungamo
Imaam Bayhaqi (rahimahullah) akunena kuti: Yazid bin Abi Sufyaan (radhiyallahu ‘anhu) pamene adali bwanamkubwa wa Shaam, Asilamu adachita Jihaad ndipo adapambana, motero adapeza chuma cholanda kwa adani. Mkatikati mwa katundu ameneyo mudalinso mtsikana okongola yemwe adaperekedwa kwa msilikali wina wachisilamu ngati gawo lake. Msilikaliyu atangolandira gawo lakeli (mtsikananayu), Yazid bin …
Read More »
Alislaam Yeretsani mtima wanu potsatira chisilamu