Kapempheredwe ka Azimayi

Chilichonse cha chipembedzo cha Chisilamu chokhudzana ndi akazi chimakhanzikika pa kukhala odzichepetsa komanso wamanyazi. Pachifukwa ichi ndi pamene Chisilamu chikulamula amayi kuti azikhala m’nyumba zawo, kukhala obisika kwa amuna achilendo, komanso kuti asachoke m’nyumba zawo popanda chifukwa chenicheni pa Sharia. M’mene mkazi walamulidwira kuswali Swalah yake – kuyambira pa chovala …

Read More »

Olemekezeka Umar (radhwiyallahu ‘anhu) adzikumbutsa za Kuyankha mafunso pa Tsiku Lachiweruzo

Ngakhale Allah Ta’ala adamudalitsa Umar (radhwiyallahu ‘anhu) pokhala m’gulu la anthu khumi omwe adalonjezedwa kukalowa ku Jannah ali padziko lino lapansi, ndipo ngakhale adali khalifah wachiwiri wa Chisilamu, adali wodzichepetsa kwambiri ndikuwopa kuyankha mafunso pamaso pa Allah Ta’ala pa tsiku la Qiyaamah. Zikunenedwa kuti nthawi ina, Olemekezeka Umar (radhwiyallahu ‘anhu) …

Read More »

Kumudziwa Allah

Allah ndiye Mlengi ndi Mdyetsi wa zolengedwa zonse. Cholengedwa Chilichonse , ngakhale milalang’amba, dzuŵa, nyenyezi, mapulaneti, kapena nthaka ndi zonse zili m’menemo, ndi zolengedwa za Allah. Munthu amene amasinkhasinkha ndi kusakasaka za ukulu ndi kukongola kwa zolengedwa zonsezi angalingalire bwino lomwe ukulu ndi kukongola kwa Amene adazilenga! Allah akutiitanira m’Qur’an …

Read More »

Qa’dah ndi Salaam

9. Osatsitsa kapena kugwedeza mutu pamene mukupanga salaamu. 10. Tembenuzirani nkhope yanu mbali zonse ziwiri moti amene ali m’mbuyo mwanu athe kuona tsaya lanu.[1] 11. Werengani mawu oti اَسْتَغْفِرُ الله katatu pambuyo pa salaam.[2] 12. Pangani ma dua popeza iyi ndi nthawi yoyankhidwa ma dua.[2] 13. Werengani Tasbeeh Faatimi kutha …

Read More »

Hazrat Ali (radhwiyallaahu ‘anhu) Akufuna Kukumana ndi Allah Ta’ala ndi zochita za Hazrat Umar (radhwiyallaahu ‘anhu)

Olemekezeka Abdullah bin Abbaas (radhwiyallaahu ‘anhuma) akunena kuti: Ndinalipo pa nthawi yomwe mtembo wa Umar (radhwiyallahu ‘anhu) unkaikidwa pa Jeneza ataphedwa. Anthu anayamba kuthamangira pamene padali thupi lake. Pamene ankayembekezera kuti mtembo wake utulutsidwe ndi kuikidwa m’manda, iwo ankawerenga durood kumfunira zabwino Rasulullah (swallallaahu ‘alayhi wasallam) ndikumamupemphera Umar (radhwiyallahu ‘anhu). …

Read More »

Qa’dah ndi Salaam

5. Ngati ukuswali rakaah zitatu kapena zinayi kenako ukamaliza kuwerenga tashahhud m’qa’dah yoyamba, nawenso werenga swalaah alan Nabi (durood). Powerenga Swala ya alan Nabi (durood), اللهم صل على محمد  werengani mpaka dzina lodalitsika la Mtumiki (swallallahu alaih wasallam) Kenako imirirani rakaah yachitatu. Musapange dua pambuyo powerenga Swalaat alan Nabi (durood).[1] …

Read More »

Chisangalalo cha Hazrat Umar (Radhiyallahu ‘anhu)

Olemekezeka Umar (Radhwiyallaahu ‘anhu) adanenapo nthawi ina kwa olemekezeka Abbaas (Radhwiyallahu ‘anhu) (amalume a Rasulullah (Swallallaahu ‘alayhi wasallam)) kuti: “Ndidakondwera ndi Chisilamu chanu kuposa Chisilamu cha abambo anga chifukwa Chisilamu chanu chidabweretsa chisangalaro chochuluka kwa Rasulullah swallallahu ‘alaihi wasallam) kuposa Chisilamu cha bambo anga. (Sharhu Ma’aanil Aathaar 3/321)

Read More »

Tafseer Ya Surah Nasr

بِسْمِ اللَّهِ الرَّحْمَٰنِ الرَّحِيمِ إِذَا جَاءَ نَصْرُ اللَّهِ وَالْفَتْحُ ‎﴿١﴾‏ وَرَأَيْتَ النَّاسَ يَدْخُلُونَ فِي دِينِ اللَّهِ أَفْوَاجًا ‎﴿٢﴾‏ فَسَبِّحْ بِحَمْدِ رَبِّكَ وَاسْتَغْفِرْهُ ۚ إِنَّهُ كَانَ تَوَّابًا ‎﴿٣﴾‏ (Oh Muhammad (Swallallaahu ‘alayhi wasallam)) Kukadzafika chithandizo cha Allah Ta’ala ndi kupambana (kugonjetsa Makka Mukarramah) ndipo ukadzawaona anthu akulowa mu Dina ya Allah ali ambiri, choncho lemekeza ndi kutamanda Mbuye …

Read More »

Qa’dah ndi Salaam

1. Pambuyo pa sajda yachiwiri ya rakaah yachiwiri, khalani tawarruk kutanthauza kukhala ndi thako lakumanzere ndikutulutsa phazi lakumanzere pansi pa mwendo wakumanja. Phazi lakumanja likhale lowongoka ndi zala ziyang’ane kuchibla. Chidziwitso : Kukhala m’malo a tawarruk kumagwiranso ntchito pa swala yomwe ili ndi qa’dah imodzi mwachitsanzo rakaah ziwiri ndi qa’dah …

Read More »

Rakaah Yachiwiri

1. Mukamanyamuka pa sajdah, choyamba nyamulani chipumi ndi mphuno, kenako zikhato ndikumalizira mawondo. 2. Pamene mukuimirira Rakah yachiwiri, tsamizirani manja anu pansi uku mukuimilira.[1] 3. Pitirizani rakaah yachiwiri monga mwachizolowezi (kupatula Dua-ul Istiftaah simudzaiwerenga).[2] [1] وإذا أراد القيام من السجود أو الجلوس اعتمد بيديه معا على الأرض ونهض ولا أحب …

Read More »