Chikondi cha Hazrat Abu Bakr (radhwiyallahu ‘anhu) Kugwirizana ndi Chikondi cha Rasulullah (Sallallahu ‘alaihi wasallam)

Bambo ake a Hazrat Abu Bakr (radhwiyallahu ‘anhu) atalowa Chisilamu. Hazrat Abu Bakr (radhwiyallahu ‘anhu) adalankhula kwa Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wa sallam) kuti: “Ndikulumbirira amene anakuikani m’choonadi! Ngakhale ndiri mchisangalaro kuti bambo anga alowa chisilamu, ndikadakhala osangalala kwambiri zikanakhala kuti omwe alowa chisilamu ndi amalume anu Abu …

Read More »

Olemekezeka Abu Bakr (Radhwiyallahu ‘anhu) amutumikira Rasulullah (Swallallaahu ‘alayhi wasallam)

Hazrat Abu Bakr Siddeeq (Radhwiyallaahu ‘anhu) akusimba motere za ulendo wa Hijrah ndi Rasulullah (Swallallaahu ‘alayhi wasallam): Tinayenda mofulumira usiku wonse ndi gawo lina la tsiku lotsatira mpaka kutentha kwamasana kunakula kwambiri. Kenako ndinapeza kuti mseu mulibe munthu aliyense woyendamo. Ndinayang’ana kutsogolo kuti ndione ngati ndingapeze mthunzi uliwonse kuti tibisalemo. …

Read More »

Ruku Ndi I’tidaal

6. Onetsetsani kuti manja asungidwa kutali ndi thupi.[1] 7. Lankhulani katatu kapena nambala yosagawanikana.[2] سُبْحَانَ رَبِّيَ الْعَظِيمِ Walemekezeka Mbuye wanga, Wamkulukulu. 8. Pambuyo powerenga tasbeeh, imirirani kuchokera ku rukuu uku mukunena tasmee:[3] سَمِعَ اللهُ لِمَنْ حَمِدَهُ Mulungu amamva amene Wamtamanda. 9.Kwezani manja (monga momwe tafotokozera mu takbeeratul ihraam) ndipo ikani …

Read More »

Ulemu wa Hazrat Abu Bakr (Radhiyallahu ‘anhu) kwa Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wasallam) ndi chikondi cha Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wa sallam) pa Iye

Pa nthawi ya Fat-he-Makkah Mukarramah (Kugonjetsa Makka Mukarramah), Hazrat Abu Bakr (Radhwiyallahu ‘anhu) adabweretsa bambo ake, Abu Quhaafah, kwa Rasulullah kuti akalowe Chisilamu. Pa nthawiyo Abu Quhaafah adali ndi zaka zoposa 90 zakubadwa ndipo adali atasiya kuona. Atadza kwa Mtumiki (Swallallaahu ‘alayhi wasallam), Mtumiki (Swallallaahu ‘alayhi wasallam) adamuuza Hazrat Abu …

Read More »

Ruku Ndi I’tidaal

1. Mukamaliza kuwerenga Surah Faatihah ndi surah ina, yimani kaye pang’ono ndipo kenako kwezani manja anu (monga momwe tafotokozera mu takbeeratul ihraam) uku mukunena takbira ndi kupita pa rukuu.”[1] Zindikirani: Takbeeraat intiqaaliyyah (takbira yomwe imanenedwa posuntha kuchoka ku kaimidwe kena kupita ku kena) iyenera kuyambika munthu akangoyamba kusuntha kupita ku …

Read More »

Munthu Wabwino Kwambiri pa Ummah uwu

Hazrat Abu Dardaa radhiyallah anhu wanena kuti: “Nthaŵi ina yake, Mtumiki (Swallallaahu alaih wasallam). adandiona ndikuyenda kutsogolo kwa Hazrat Abu Bakr (Radhiyallahu ‘anhu) “Pamene Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi wa aalihi wa sallam) adaona izi, adandiuza kuti: “Usayende kutsogolo kwa amene ali wabwino kuposa iwe. Pambuyo pake Mtumiki (Swalla Allaahu ‘alayhi …

Read More »

Kulemba Durood pa kutha kolemba dzina la Mtumiki swallallahu alaih wasallam

عن أبي هريرة قال: قال رسول الله صلى الله عليه وسلم: من صلى علي في كتاب لم تزل الملائكة تستغفر له ما دام اسمي في ذلك الكتاب (المعجم الأوسط للطبراني، الرقم: 1835، وسنده ضعيف كما في كشف الخفاء، الرقم: 2518) Olemekezeka Abu Hurairah (radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (swallallahu alaih …

Read More »

Qiyaam

12. Kenako udzayamba kuwerenga surah Faatihah ndi surah ina kapena gawo lina la Quraan Majeed. Musanayambe kuwerenga surah faatihah, werengani tasmiyah chifukwa ndi gawo la surah fatihah. Tasmiyah ndi kuwerenga: بسم اللهِ الرَّحْمنِ الرَّحِيمِ M’dzina la Allah, Wachifundo chambiri, Wachisoni. Dziwani izi: Ngati ndiwe Imaam, werenga tasmiyah mokweza mu Swalaah …

Read More »

Hazrat Abu Bakr Siddeeq (Radhwiyallahu ‘anhu) ali m’phanga la Thaur

Ali kuphangako paulendo wa Hijrah, zikunenedwa kuti Hazrat Abu Bakr Siddeeq (radhwiyallahu anhu) adali ndi nkhawa kuti palibe cholengedwa chomwe chingatuluke mu dzenje lililonse la mphangamo ndi kuvulaza Hazrat Rasulullah (Swallallaahu ‘alayhi wasallam). Choncho, anayamba kutseka mabowo onse a m’phangamo ndi zidutswa za malaya ake apansi. Komabe, padali mabowo awiri …

Read More »

Tafseer of Surah Kauthar

Ndithu, Ife takupatsa (ndi kukudalitsa) zabwino zambiri Choncho pemphera Swala kwa Mbuye wako, ndipo pereka nsembe. Ndithu, amene akudana nawe adzadulidwa.

M’surayi Allah Ta’ala akulankhula ndi Mtumiki (Swallallaahu ‘alayhi wasallam) kuti: “Ndithu, Ife takupatsa (ndipo takudalitsa ndi) zabwino zambiri.

Zabwino zochuluka zomwe Hazrat Rasulullah (Swallallaahu 'alayhi wasallam) adadalitsidwa nazo padziko lapansi zikuoneka kudzera mu dzina lake la Mubaarak ndi kukwezedwa ulemu, chipembedzo chake chikupitilira kutukuka ndikukula mphamvu ndi mphamvu, ndi kuchuluka kwa anthu olowa m'chipembedzo cha Allah. Chisilamu chikuchuluka tsiku ndi tsiku.

Read More »