Qiyaam

10. Mukangoiyamba swalah yanu werengani Duaa-ul Istiftaa chamuntima. وَجَّهْتُ وَجْهِيَ لِلَّذِيْ فَطَرَ السَّمَاوَاتِ وَالْأَرْضَ حَنِيْفًا مُسْلِمًا وَمَا أَنَا مِنَ الْمُشْرِكِيْنَ إِنَّ صَلَاتِيْ وَنُسُكِيْ وَمَحْيَايَ وَمَمَاتِيْ لِلّٰهِ رَبِّ الْعَالِمِيْنَ لَا شَرِيْكَ لَهُ وَبِذلِكَ أُمِرْتُ وَأَنَا مِنَ الْمُسْلِمِيْنَ Ndikuyang’ana nkhope yanga kwa Yemwe adalenga thambo ndi nthaka, ndikukhala panjira yoongoka popanda kusokonekera, …

Read More »

Olemekezeka Abu Bakr (Radhwiyallahu anhu) Kupereka Chuma Chake Kwa Mtumiki (Swallallaahu ‘alayhi wasallam)

Olemekezeka Abu Hurairah (radhwiyallahu anhu) akusimba kuti Mtumiki (swallallah alayhi wasallam) adati: “Palibe chuma cha munthu chomwe chidandipindulira monga chuma cha Abu Bakr (radhiyallahu anhu), atamva izi olemekezeka Abu Bakr (radhwiyallahu anhu) adayamba kulira nati: “Chuma changa ndi zonse ndi zanu. Pali nkhani ya olemekezeka Abu Hurairah (radhwiyallahu anhu) m’buku …

Read More »

Kuwerenga Durood Musanapange Dua

عن عبد الله بن مسعود قال إذا أراد أحدكم أن يسأل فليبدأ بالمدحة والثناء على الله بما هو أهله ثم ليصل على النبي صلى الله عليه وسلم ثم ليسأل بعد فإنه أجدر أن ينجح (المعجم الكبير للطبراني، الرقم: 8780، ورجاله رجال الصحيح إلا أن أبا عبيدة لم يسمع من أبيه …

Read More »

Qiyaam

7. Nthawi yowerenga Takbiiratul ihraam (Takbiir-e-Tahriimah) onetsetsani kuti maso anu a kuyang’anaya malo opanga Sajdah ndikupendamitsa mutu wanu pang’ono pansi.[1]  8. Ikani dzanja lanu lamanja pa dzanja lanu lamanzere ndikuwaika pansi pa chidali pamwamba pa nchombo.[2]  9. Gwirani joini yanu ya dzanja lamanzere ndi dzanja lanu lamanja, zala zanu zakumanja …

Read More »

Chikondi cha Hazrat Anas bin Nadhr pa Hazrat Rasulullah (swallallahu alaih wasallam) Kuphedwa ku Uhud

Pamene Asilamu adagonjetsedwa ku Uhud, mphekesera zidayamba kufalikira kuti Sayyiduna Rasulullah (swallallahu alaih wasallam) waphedwa. Nkhaniyi idawapangitsa ambiri mwa ma Swahaabah kutaya mtima ndi kutaya chiyembekezo. Sayyiduna Anas bun Nadhr adawona Hazrat Umar ndi Hazrat Talhah pamodzi ndi gulu la ma Sahaabah ali mu chisoni chachikulu ndi kutaya mtima. Iye …

Read More »

Tafseer Ya Surah Ma’un

Kodi mwamuona amene akukana (za tsiku la) Chiweruzo? iye ndi Yemwe akukankha (ndi kutsekereza) wa masiye, ndipo salimbikitsa Kudyetsa osauka. Mavuto akulu ali kwa amene akuswali, amene akunyalanyaza Swalah yawo. Iwo amene (amachita zabwino) podzionetsera, ndipo amakana kupereka (kapena kubwereketsa) ziwiya zawo ngakhale zinthu zazing’ono (zomwe anthu akuzifuna).

Read More »

Answaari wina agwetsa nyumba pansi

Tsiku liina Hazrat Rasulullah (swallallahu alaih wasallam) ankadutsa mumsewu wa Madinah Munawwarah pamene adawona nyumba yomwe inali ndi dome. Adafunsa kwa Swahaabah. “Ichi ndi chiyani?” Anamuuza kuti inali nyumba yatsopano yomangidwa ndi mmodzi wa ma Ansaar. Hazrat Rasulullah (swallallahu alaih wasallam) anakhala chete. Tsiku lina, Answaari amene adamanga nyumbayo adadza …

Read More »

Kuwerenga Durood musanapange Dua

عن فضالة بن عبيد قال: بينا رسول الله صلى الله عليه وسلم قاعد إذ دخل رجل فصلى فقال: اللهم اغفر لي وارحمني فقال رسول الله صلى الله عليه وسلم: عجلت أيها المصلي إذا صليت فقعدت فاحمد الله بما هو أهله وصل علي ثم ادعه قال: ثم صلى رجل آخر بعد …

Read More »

Qiyaam

1. Pamene mukufuna kuswali, imani ndi kuyang’ana pa Qiblah.”[1] 2. Poimirira kuti muswali, imani molemekeza kwambiri. Yang’anizani mapazi onse ku Qiblah ndipo sungani mpata wa pafupifupi dzanja limodzi pakati pawo. Poswali pagulu, ongolani masafu (mizere) ndipo imani moyandikana momwe mungathere, popanda kusiya mipata pakati panu. Mapazi sayenera kupatukana m’njira yakuti …

Read More »

Hazrat Bilaal (Radhiya Allaahu ‘anhu) pa imfa yake

Pamene Hazrat Bilaal (Radhiya Allaahu ‘anhu) adatsala pang’ono kumwalira, mkazi wake adayamba kunena kuti: “Ha! Ndi zomvetsa chisoni bwanji! Mukuchoka m’dziko lino!” Hazrat Bilaal (Radhiya Allahu anhu) anayankha kuti: “Zili zokondweretsa ndi zosangalatsa kuti mawa tikukakumana ndi abwenzi athu, tikakumana ndi Muhammad (Swalla Allaahu ‘alayhi wa sallam) ndi maswahaba ake.”

Read More »